Umu ndi momwe a Prophet Bushiri adapezera ndalama, za dziwika
Вставка
- Опубліковано 8 жов 2024
- A Bushiri ndi munthu olemera kwambiri mu dziko la Malawi komanso Africa. Iwowa pamanveka mphekesera zosiyanasiyana zokhudza chuma chawo. mu video iyi tikuona momwe iwowa adapezera chuma chawo.
Check magazine website: 265entmag.live/
Radio Website : radio.265entma...
Company website: agency.265entm...
Pastor wasatana ameneyo osati wa mulungu ai komaso mboliyamake munthu oipa ameneyo mukamadya ndalama za ameneyo chifukwa cha umphawi umphawi wanu sudzatha vomelezani kukhala mphawi koma ndalama za bushili musalandire
Makolo ake sizikuwakhuza amakana anything from him akuvutika kwaoku fukwa akuziwa kt mwana wao sali straight
Mmmmmmmmmh no comment only God knows
akufuna attention ku channel yake,😮😮😮
@@alicembetewa5151 ndichifukwa timatulutsa content
Mukudziwa ndinu mukunenanu😂😂😂😂
Simunthu wa mulungu Uyo
The truth is with him and God we have no idea 🙌
Only GOD knows
Bushiri akufuna kuno ku South Africa waba kwambiri ziko lino.
Ndi njoka iiii inu simunthu akudikilira moto awa jahena
Akulu inu ngabonza
Machende ako kulimbikisa usatanc
Only God knows
iwee uyu ndi wa satanic not izoo ukunama akupasa zingati kodi uzindifunsa ine bwino uwoneka anakupasa ndalama
Mmodzi mwa anthu osaziyanganirani pansi kuno kumalawi.
WAKUBA ALIBE MALEMB MBA PROGRAM YOU SO 😢
Akudziwa ndi mulungu
Mulungu yekha ndiye odzuwa zonse
Inu koma inu Satan uyu inu osamati prophet
osamangofuna kutchuka kuti mumaulutsa nkhani palibe chanzeru apa
Zopusa
Watani munthuwu ndiolimbikira musiyine mukufuna kuziwa kumene anakatenga ndarama buzi nose musiyeni ndiolimbika