BON KALINDO WANG'ALULA DR MICHAEL USI LERO__28 January 2025

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 123

  • @alexanderchamgwera-jm1qy
    @alexanderchamgwera-jm1qy 9 днів тому +7

    Nonse amene mukumunyoza kalindo nzeru mulibe mwanva izizi ananena kale usi ndendaninso kufupika kwake

  • @JasonMailos
    @JasonMailos 5 днів тому

    ❤❤❤❤❤ manganya NDI amene anampha chilima

  • @AishaLeman
    @AishaLeman 9 днів тому +7

    Mr kalindo,my boss❤

  • @AggieKwekwesa
    @AggieKwekwesa 9 днів тому +4

    Bonie kalindoooo the DC❤

  • @OscarChimkwende
    @OscarChimkwende 9 днів тому +5

    Koma anthu amene amadana ndi uyu kalindo mutu wake sumagwira chifukwa chomwe wakamba chimachitika kupita kwanthawi iweyo kalindo ndikatundu

  • @austinenaaman
    @austinenaaman 9 днів тому +5

    Tikavotere Dan Mahata bas😊

  • @TroubleJames-c8p
    @TroubleJames-c8p 8 днів тому +1

    The DC big mn I lov u mumKonda malaw

  • @ChrisKadzuwa
    @ChrisKadzuwa 3 дні тому

    Akalindo mukunene zoona. Munthuyu alibe mzeru

  • @Edward-y3v
    @Edward-y3v 9 днів тому +2

    Malawi hope ndi Denis mahata

  • @mairosvicmasamba7922
    @mairosvicmasamba7922 9 днів тому +8

    Give him a chance He has right to do wht he is able to do ..

  • @LimzeySande-b9n
    @LimzeySande-b9n 9 днів тому +2

    Kalindo is Good guys chirungamo ichi Big

  • @lewisdicksonmlozi130
    @lewisdicksonmlozi130 9 днів тому +1

    Guys tiyeni tisethe dziko lathu tivole.. Denis mahata

  • @HasheemSalade
    @HasheemSalade 9 днів тому +2

    Usi sangaputsitse anthu ndi mwana wang'ono kwabas

  • @alexmalunga8896
    @alexmalunga8896 8 днів тому +1

    Manganya sangamve chisoni chifukwa ndi obwela ku Malawi he from Zimbabwe.mulungu atithandize

  • @CassimAbudallah-s9h
    @CassimAbudallah-s9h 8 днів тому

    THE DC U THE MAN IN TOWN

  • @AmunaMisso
    @AmunaMisso 2 дні тому

    Koma ndipo kukonda ndalama muthu was mai

  • @ChilinguloRobert
    @ChilinguloRobert 9 днів тому +1

    He is an excellent new rebrand. Let's support him to be a DPP member.

  • @BenMbewe-id8ok
    @BenMbewe-id8ok 7 днів тому

    Ukaseka nanenesa ndimaseka ndimawona ngati kukuseka ndikuwujeni😂😂😂

  • @AnnieKachere-qu5yy
    @AnnieKachere-qu5yy 3 дні тому

    Inenso namva chisoni kwambiri kuti Koma izizi ndi zoona?

  • @WatsonMtegha-r1c
    @WatsonMtegha-r1c 9 днів тому +2

    Ndazindikira kuti Bonikalindo ndimuthu oipa wosafunira anzake zabwino! Zomwe usi akuchita moti sakuona ndithu? Eeee ambambo inu takuzindikirani ndithu.

  • @DennisShane-ql5er
    @DennisShane-ql5er 9 днів тому +1

    Asogoleni akumalawi ndiyovesa Chisinau kwambili

  • @MartinNice-z9n
    @MartinNice-z9n 8 днів тому

    The DC respect cz umanena reality before action

  • @MimisellaSiska
    @MimisellaSiska 7 днів тому

    Ife bola angotitchenetsa nsalu zo iya ,zikatitopesa tizipanga matewera

  • @HappyNyasulu-i8d
    @HappyNyasulu-i8d 10 днів тому +3

    Usi ndi wa mcp

  • @FelixKChisale
    @FelixKChisale 10 днів тому +1

    Akalindo inu mumafunakut dr usi akutsatileni ku chipani cha dpp kwanuko

  • @BrevassTherah
    @BrevassTherah 8 днів тому

    Mbuzi iyiyi siyizatheka yisiyeni yizilubwalubwa,

  • @ErickCPatrick
    @ErickCPatrick 9 днів тому +1

    sizingachititse,kt,mcp,ilize,zimenezo,fundo,mulibe,kumango,bweleza,zimodzimodzizo,,km,awawa,anthu,moti,akakuvotenleeni,fundozake,zimenezo,

  • @BenMbewe-id8ok
    @BenMbewe-id8ok 7 днів тому

    Kodi awa apenga liti
    Anthu adyela zawavuta palibe akuwadyetsela nde misala ikuwathamangitsa pompano tiva

  • @LimbikaniTambala-z1y
    @LimbikaniTambala-z1y 9 днів тому +3

    Ine ndiye ndi pambuyo Dr Usi

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 9 днів тому +1

    Manganya, ati waumba nsalu yake, ati asokoneze DPP ndi UTM ati wodya zake alibe mlandu ati kuonetsa nzeru zake zakufupika ngati ndondocha.
    Manganya uchenjere unaphetsa chilima ndicholinga kuti ukhale pamenepo.
    Manganya ndimagwila pakhosi tsiku lina

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 9 днів тому

    Munthu ukayambisa chipani zina lachipani limakala losiyana ndichipani chimene unali. Sitipanga makaka ofanana ndi chipani chomwe unali ndiye golden simokoyo muziwe kuti ndifiti yoopsa kwambiri kuthekaso kuti mwina ndiye anagwesa ndege kuti atenge makakawo fiti yimawonekera poyera ngati munthu waphayo sanali olakwa

  • @ChristopherCk-s4w
    @ChristopherCk-s4w 8 днів тому

    Wabodza lwe umakhara mbali ya dpp timakudziwa lwe munthu opanda sogolo

  • @mcfarlenmatope4138
    @mcfarlenmatope4138 9 днів тому +1

    kuswa kuswa Kalindo.... tiyenazo....kkkkkk

  • @AlicksonGoliath
    @AlicksonGoliath 8 днів тому

    Iwe osayambitsa chipani chako bwanji?,munthu mwamuthamangitsa ku chipani ndiye mumati atani?,

  • @AmandaConstance-fx8cr
    @AmandaConstance-fx8cr 9 днів тому

    Koma kumalawi eeeeeeeee Kaya mwe 😢😢😢😢😢😢

  • @GiftManda-w5l
    @GiftManda-w5l 8 днів тому

    Respect

  • @ChembeWaimba
    @ChembeWaimba 9 днів тому

    DC mutu sukugwira, munthu uyu wabalalika zokamba zatha wayima mutu

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 10 днів тому +1

    Vuto ndi chani nanuso akalindo usi ndi ufulu wake nsa je pela

  • @ChettoSongeah
    @ChettoSongeah 9 днів тому

    kma usi ngati amalephela MP kudela lakwawo ndye upule anukhapo

  • @md.ruhul-aminmd.ruhul-amin298
    @md.ruhul-aminmd.ruhul-amin298 10 днів тому +1

    The Dc

  • @DesireMoyo-y8x
    @DesireMoyo-y8x 9 днів тому

    Zinayamba ndikale
    Udf inachoka mu mcp
    Dpp inachoka ku udf
    Pp inachoka mu dpp
    Utm mudpp
    Pdp inachokaso mu dpp
    Chachilendo ndichani
    Aliyense pamalo pake mulungu alamula yekha pa 16

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 9 днів тому +1

    Michael Usi is exercising his democratic right. What’s your problem? Komanso mesa UTM inapinyulitsidwa ku DPP

  • @PatriciaAlomwe-oz8wc
    @PatriciaAlomwe-oz8wc 9 днів тому +3

    Mpaka kuvotera odya zake alibe mulandu kkkkkk ndiye kusokeratu

  • @IntakeSpillway
    @IntakeSpillway 9 днів тому +1

    Munthu anachita kuchotsedwa apa muli kukamwa wawawa mxiew

  • @JamesChiphazi
    @JamesChiphazi 9 днів тому

    Mcp gwilizano ndi odya zake alive milandu ,,,,, apano maula aathu amwe anali pa upo ogwesa ndege aja mwaagwilatu mupangaso kafukufuku wina ngati

  • @CharlesJames-f1w
    @CharlesJames-f1w 9 днів тому

    Opepera.akolo.ndioopwe.kwambiri

  • @GrecianSeveli
    @GrecianSeveli 9 днів тому

    Tiuze zoveka iwe ulibe zeru iwe uzawerukira yomweyo

  • @graciousmtonga6522
    @graciousmtonga6522 9 днів тому

    A Kalindo inuyo yambisani Chanu Chipani basi muzachite zokhozeka enawa alephera kale..ndikale munayamba kubwebweta Lija asàaaa .Tizakuvoterani
    Manganya has a right as a Malawian Citizen kuyambisa chipani as everyone Malawian Can do

  • @muhamadizaidiphiri4449
    @muhamadizaidiphiri4449 9 днів тому

    Kalindo sanyengelala munthu bwino wa kalindo saopa munthu

  • @AMONINICHOLAS-g2m
    @AMONINICHOLAS-g2m 9 днів тому

    Koma zoti mudziwe ndizakuti, Kalulu sangathe kumwamadzi Galu alipambuyo, 😢😢 mwimvi oyang'anila umatosa mmaso,, Bawo ikakutha dziwa kuweya Ina msanga ndiyo khani imeneyo

    • @RajaMakawa-q1y
      @RajaMakawa-q1y 8 днів тому

      Tikavote mwaa unyinji bs Mr chikangawa achoke bs

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 9 днів тому

    Manganya chinangofupika ngati chindondocha that's why pali sign ya khasu pansalu yomwe wapanga. Ndindondocha manganya

  • @EdwardRichman-zs5pl
    @EdwardRichman-zs5pl 6 днів тому

    Kd utm inachokela kt nde odya zake alibe mulandu popanga zake Mesa ndufulu iwe ndi mbuzi kwambiri mphuzilako kupanga zako

  • @jomochirwa
    @jomochirwa 9 днів тому

    Ameneyi ndi amene watenga 80 percent yonse ya utm.tsono poti aliyense ali ndi ufulu woyambitsa chipani chake basi musiyeni ,inuso mutha kuyambitsa chanu.

  • @ChrispinKashosha
    @ChrispinKashosha 9 днів тому

    Bas vomelezani inu kut mzanu ndiwazelu kusiyana ndiwe

  • @LichardMuleva
    @LichardMuleva 8 днів тому

    Nom

  • @makhalidwemclean1987
    @makhalidwemclean1987 9 днів тому

    Malawi mulungu amalikonda keno malawi ndi dziko lotembeleredwa,tigwire ziti.

  • @morsonmhone
    @morsonmhone 9 днів тому +3

    Bon kalindo mutu umamuvutitsa . I think misala imamubvutitsa. Dr Usi bravo! Inayi ndi misala isakusokonezeni

  • @CharlesJames-f1w
    @CharlesJames-f1w 9 днів тому

    Amanena.chocho.amalawi.inde.big❤

  • @JamesSinyolo
    @JamesSinyolo 9 днів тому

    Kodi manganya abwelera liti kwawo ku Zimbabwe

  • @shotsfired588
    @shotsfired588 9 днів тому +2

    Achisilu awa, chisale anabera dziko ma billions omwe anakamangira ma school ndi zipangizo za chipatala koma awa achisilu awa kupita ku khothi kukachemerera mbava ngati chisale. Mmesa umadana ndi katangale. Mbuzi ya munthu iyi. Osamumvera uyu akukonza tsogolo lake.

  • @muhamadizaidiphiri4449
    @muhamadizaidiphiri4449 9 днів тому

    Adamuphesa chilima ndi USI

  • @mabvutomichaelpanagona1949
    @mabvutomichaelpanagona1949 9 днів тому +3

    Michael usi anamuchotsa ku UTM chifukwa cha uchitsiru manganya ndi wopusa kwambiri

    • @ChipiliroMsanyama
      @ChipiliroMsanyama 9 днів тому

      @@mabvutomichaelpanagona1949 wopusa ndi iwe ulichaani tamuwoneni Ali mbu

  • @DemusterKamwimbi
    @DemusterKamwimbi 9 днів тому

    Koma usi akunama mcp yawanamizi dziwani skc mzmu wake udzakatha wina aliyense

  • @MollenMponya
    @MollenMponya 7 днів тому

    Iwe ulibe abale anamwalira Kuti uziwakumbukira

  • @BlessingsSaidi-h3g
    @BlessingsSaidi-h3g 9 днів тому

    D C

  • @ThomasMaxwell-ks7yi
    @ThomasMaxwell-ks7yi 9 днів тому +2

    Munthu anamuchotsa mmati atani munthu amadya msima mwana wake atamwalila siyani jelas

  • @GrecianSeveli
    @GrecianSeveli 9 днів тому

    Garu kobasi

  • @KhalidweFelix
    @KhalidweFelix 8 днів тому

    😂Ma battery ati

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 9 днів тому

    Munthu kuti muziwe kuti zeru alibe choyamba amakhala wamakani sa ava za wina. Amakhala osata mapazi azake kwambri . Amapanga zinthu mwachibisira. Amalimbana kutenga zayeni ndikukhala zako. Munthu wotere ndimunthu wakhaza moopsa.

  • @WangaPhiri
    @WangaPhiri 9 днів тому

    Nde usi walakwa Chan? Asayambitse chipan chifukwa chot pangotha 7 months chigweren ndege, nde iye asapange zake chifukwa cha malem anuo? Komaso munthu anachita kumchosa mu chipan nde azipangaso za UTM chifukwa Chan, komaso munthu akafa wafa olo mpite where he died siziphula kanthu.

  • @PatrickMisomali-v6q
    @PatrickMisomali-v6q 9 днів тому

    Namanyenga mpaka kuyambitsa chipani koma ndie uwathatu akazi kumeneko

  • @HarlodLemwe
    @HarlodLemwe 8 днів тому

    iweo ukatero zako zimakhala zaayela uzipusisa anthu kwanu komweko ngat dziko lino likuvutika iweo ukuchitapo chani ngat zimakukhuza?

    • @FracksonNserebo-e6s
      @FracksonNserebo-e6s 8 днів тому

      Km zomwe akulakhulazi analakhukapo ndipo apa ndi izi zachitikazi
      So do you think he is lying

  • @PatriciaAlomwe-oz8wc
    @PatriciaAlomwe-oz8wc 9 днів тому

    Golden smoke the DC sopano kkkk

  • @MilikaKilion-tn1bn
    @MilikaKilion-tn1bn 10 днів тому +3

    Malawi ndi ovesa chisoni to be honest we are not serious

  • @Molsonabdul
    @Molsonabdul 9 днів тому

    Mesa ndi zako

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 10 днів тому

    Mkunena zamavoti komaadpp akupha anthu akakhala wamcp simyankulapo kod ufulu umene mkumenyela wa anthu adpp wokha okha enawa sianthu zisilu inu komaso afiti inu anthu akumwela

    • @Emelzelie
      @Emelzelie 9 днів тому

      Anthu Ake ati akupha a DPP?? Ndege ija anagwetsa ndi a DPP, mavuto waku BT uja simunapha nokha mkumanamizira azanu. Ngt anapha a DPP y sakumangap aliyese until now

  • @ChipiliroMsanyama
    @ChipiliroMsanyama 9 днів тому +1

    Born ndi kapena uyu

  • @InnocentKalua
    @InnocentKalua 10 днів тому

    Mbambande

  • @morsonmhone
    @morsonmhone 9 днів тому

    Ndipo ulira sunati, dikila iwenso SI alipo omwe amakutuma? Sunati ulila

  • @WilliamMasula-cb1mg
    @WilliamMasula-cb1mg 9 днів тому +1

    Mr Bon Kalindo mudasankha kukhala actist and leave Micheal Usi alone for what he's doing

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 9 днів тому

    SIX MONTHS KUYAMBITSA CHIPANI NDIYE ANTHU ACHIKODE ZOONA KOMA MWAZI WA MUNTHU aa NDIOOPSYA NDITHU 😭😭

  • @ShakiraJackson-x8w
    @ShakiraJackson-x8w 9 днів тому

    Kodi kumalawiku kulibe limitation ya zipanizi kamalawi Kang,Ono ng,Ono mpaka ziphani 100 wina aliyense amene walota ndi manthongo thoo kuyambitsa chipani ayi tsuka man

  • @bliksempiemoerdyk6605
    @bliksempiemoerdyk6605 9 днів тому

    Zipani zonsezo Za chiyani kd

  • @justinmalala-e4o
    @justinmalala-e4o 9 днів тому

    Koma penapake zipani zotsutsa zomwe zili mdziko muno ndizozizila, zofoila

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 10 днів тому +4

    Kuswa Kuswa Golden smoke, Bon kalindo mwana oopsa kwambiri 🎉🎉🎉

    • @gwatandingo9502
      @gwatandingo9502 10 днів тому

      Kalindo alibe zelu Muthu amuchotsa amafuna apange bwanji 😂😂😂😂😂

    • @MisheckAselo
      @MisheckAselo 9 днів тому

      @gwatandingo9502 iweyo ndiye wamzeru 🤭🤭🤭

  • @Bbbbwesgtcjoug
    @Bbbbwesgtcjoug 9 днів тому

    Eya ayambitse vuto palibe iwenso yambitsa chako chotukaana opposition simukuwina umbuni ndi umenewu usi ♥️♥️❤️🙏 wonetsa ufulu wako MCP my vote ❤️❤️❤️😊😊

  • @goodsonkhulani7470
    @goodsonkhulani7470 10 днів тому

    😂😂😂ndaitchelatu

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 10 днів тому +6

    Mbali yanga sindikuwonapo vuto pamenepo koma sanje chabe 😂😂😂😂😂

  • @HarlodLemwe
    @HarlodLemwe 8 днів тому

    kunali azanu pano ali kut zaziiii

  • @henryhenry6632
    @henryhenry6632 10 днів тому

    Iwe kapolo, kayambitse chako chipan dzimachende dzako

    • @MussaAli-h4i
      @MussaAli-h4i 9 днів тому

      Iweyo uli ND mango 🥭 ulibe machende

  • @BlessingKamanga-v9f
    @BlessingKamanga-v9f 10 днів тому +2

    Michael USi anachotsedwa mu UTM ndiye mumafuna apange chani. A Bon Kalindo mwangokhala ndi nsanje

  • @RonneckKhamula
    @RonneckKhamula 9 днів тому +1

    Manganizo ndi zolinga ndi zosiyana, Bon sakudana ndi aliyense akungoyankhula zomwe akuziona kuti ndi zothandiza

  • @GrecianSeveli
    @GrecianSeveli 9 днів тому

    Kkkkkk sanje iwe!!!!

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 9 днів тому

    A bon kalindo ndinu a chitsiru mzanu mwamuthamangisa mu chipani chanu nde akanatani

  • @BlessingKamanga-v9f
    @BlessingKamanga-v9f 10 днів тому

    The DC has joined DPP

  • @mdyombamw7659
    @mdyombamw7659 9 днів тому

    Zipani zoyambisa ahlomwe zokha kupitilila 10... Ehhh mutofuna chaniii😂...

  • @YusufMapata
    @YusufMapata 9 днів тому

    zosadabwitsa usi anali ndi chipani chake wodya zake alibe mulando utm yisadayambe komaso kufanana kwa mayuforomu sivuto

    • @paulbanda3028
      @paulbanda3028 9 днів тому

      Nenani fundo akalindo muti chalakwika ndi chan inuso mwa kwela team ina yake2

  • @FrankAbraham-e9o
    @FrankAbraham-e9o 9 днів тому

    Galu wa DPP Born kalindo uyuu
    Chomwe walakwa usi ndichani?

  • @AMONINICHOLAS-g2m
    @AMONINICHOLAS-g2m 9 днів тому

    Koma zoti mudziwe ndizakuti, Kalulu sangathe kumwamadzi Galu alipambuyo, 😢😢 mwimvi oyang'anila umatosa mmaso,, Bawo ikakutha dziwa kuweya Ina msanga ndiyo khani imeneyo