Timumva Kuwawa Chilima Mu 2025?
Вставка
- Опубліковано 27 сер 2024
- Fans of UTM and Right Honorable Dr. Saulos Klaus Chilima Vice President of Malawi this is for you. Enjoy! For the anyone else do you think SKC is a force to reckon with in 2025?
#nyimbozachimalawi #malawimusic
Rest easy my Guy, for once i had hope for real change. Thank you for your service
Supporting mbava Malawi style. Choncho katangale angathe ku Malawi. Nkomwenkomwe Chilima sangayime pa president as thye law forbids him.
DC Bon kalindo wanena yese akusapota mbava mchitsiru
Chilima ndi machine
Aaaaaa zokuba basi anthu mene akuvutikilama kumalawi eya
Afuna kumunamiza Chilima anthu
Bhazuka machine Dr SKC
Chilima akachoka ku Mcp , chipani chowina ndi Dpp
Chilima is not a thief, it was just a move by MCP to turnish his name So that he doesn't stand in 2025. It was well calculated by Chakwera.
Ayise Ngati ukufunya gayiwa bola usikafuna maganyu kuchomerera mbamva amwene😱😱😱😱
Chilima
Chilima mashine
Aaaaaaa koma umbuli ndikhani zina,,,kumbera mfiti m'manja
Tapelekani ma comment mukusowa chonena because the guy muli nzeru osati sewero and titamupanga kukhala president wa dziko lino ndikuuzani munthawi yochepa chabe Malawi atha kusitha tikuyenera kusiya mndale za zipani monga tinachitira muja ndikusakha omwe Ali ndi kuthekera not poti ndi wakwathu ai mkulu analakhula uja wapelekako example Chilima ali bwino ndi Pitala zinthu zimayenda bwino koma atangochoka chipwilikiti mpakana DPP inaluza boma nayoso MCP pomwe inalu ndi ubale wabwino ndi Chilima mesa tinagula fertilizer wa 4.9.99 muno pano bwanji? NDE the guy muli nzeru bad zotukukira dzikoli..abale azanga zoona mukufuna Gogo lotha ntchito LA zaka 82 litilamulire?azikangogona achina Norman Chisale azikaba ndalama, mpakana kutayilita kutisakhira munthu osadziwa chilichose Chimulirenji as vice president abale munthu ukafika zaka zimenezo umapuma orso mwiniwake ananena osakakamiza magogo kukugwilirani ntchito inuyoso munthati kuima ngati president kulibe school ya upresi 6:35 dent lamuro la age limit lija limayeneraso kupanda pass imagine the candidate Ali ndi zaka 80 nde alamulire 2 terms azakhala ndi 90 yrs are we serious ndi dziko lathuli a malawi, mavuto omwe boma iliri ladutsamo agogo aja sakanakwanitsa or pang'ono, Chilima ndi machine akatundu or kuti amene kut apanga press conference mawa ma battery awailesi mumashop amatha malo oonetsa film kudzadza meaning the guy has something special let's try him malawias
Wasowa choimba kodi, kodi chimakhala chili chain kumasapota mbavazi
sitikufuna anthu otibera misonkho yathu onse atonse alliance alibe CHOTI angatiuze ife amalawi zotinamidza ife tatopa Nanu nonse mbava zokha zokha
Zachamba chilima mwanva!!!
Chilima machine
Kuombera fiti manja mbava yeniyeni
Chilima ndiwakuba mupaka nyimbo guys
Wakuba mambo wako chakwera na pitala chilima bomaa
Kkkk mmmm koma mudziyimba kuti Chima wakubayeeeeee! Komanso wabodzasaaa, mukadzamuvotela Chilimayeee, adzabayeeee.
Kujoinana ndi MCP kuja pakokha it was a very big mistake and nkhanza that he did to Malawians.Ndiye poti aMalawi ambirife tinalodzedwa/opepela zinthu ngati zimenezi samaganizira kuti tikuvutika ku Malawi chifukwa cha decision imene iye anapanga yolibwezeretsa boma la nkhanza m'boma.Atleast akanayima payekha Kapena kujoinana ndi chipani China chake olo Aford.Koma MCP!????.Ayi ndithu people uyu mngwaphuma kwambiri uyu ndipo wa dyera musadzayelekeze kuononga vote yanunso pa uyu.God forbid
Mmmmm
Mbava
Mukufuna apitilize kuononga zakeso et gwape ameneyu angakhulupilire ndan
Zopusa mwaponya apanu mukusowa chochita😲
Km zowona zonsezi tikumvadi ukuwawatu ndi ATONSE ALLANCE
Munthu wa dyera uyu.Anatenga kuwachotsetsa achinyama ku ulamuliro wabwino wa DPP umene zinthu zinali bwino kuwapititsa ku Ng'ona za MCP.Zonsezi anapanga chifukwa cha dyera ndi Phuma ndi upresident.Only anthu akhungu mosaona patali amagomera Chilima
Akuba ngati ameneyi
Inatimvetsa kale kuwawa ameneyu tilibe naye mau.wabodza, ofowoka.
Chilima si mbamva zili ku MCP. The most effective way to destroy people is to deny and obliterate their own understanding of their history. Thats propaganda.
Munatinamiza kale inu sima yodya katu ija ilikuti munataya geme
Nokha basi
Koma ndiye mwalawilila chitukuko tinasachione ko iwe ndi mbuzi ndi thu
Kupunsa
Koma satana ndi oopsa guys eerr
Mboli zanu
Awandiopusa inu
Chilima ndi 1 palibeso make pandale mdziko mino
Amakumbukira ADAD uyu kuti anali .munthu wabwino... pano manyadxi okha okha ... ADAD ananyodxedwa kutukwanidwa kusemeredwa nyatsi koma ADAD anali pheee kumvesera .lero chilima wangoyetsa kupanga matukutuku mmmmm mcp yati aaaaa mwanayu sakuidziwa mcp ndiyesa anali mwana 1987 koma timuonese anaona Muwaro ndi Gwede .lero uyo
Koma misala ina iyi
Zaziiiiii
Uziona za Ziiii
Amene ukuyimba nyimbo yako yopusa naweso ulimugulu lambava zoopsya m.malawi muno muhanya uno munthu wanzeru zake angavotereso chilima mbava ya zuneth satar iweso ndiwe garu umanamiza dziko kuti anthu adzadya katatu azagura fertilizer 50kgs pa mtengo wa k4950 zikutheka Lero chilima ndiye munthu woyipa kwambiri 50kgs fertilizer mpaka na k90. 000 stupid foseki akagwere uko
Kkkkkkk 🔥🔥
Mbava mambo wako chakwera chilima boma
Kuchenjres akulu awa apit nazooo kumanda