Timumva Kuwawa Chilima Mu 2025?

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 27 сер 2024
  • Fans of UTM and Right Honorable Dr. Saulos Klaus Chilima Vice President of Malawi this is for you. Enjoy! For the anyone else do you think SKC is a force to reckon with in 2025?
    #nyimbozachimalawi #malawimusic

КОМЕНТАРІ • 47

  • @ndabaningichisiza9574
    @ndabaningichisiza9574 2 місяці тому +2

    Rest easy my Guy, for once i had hope for real change. Thank you for your service

  • @ephraimphiri8919
    @ephraimphiri8919 Рік тому +4

    Supporting mbava Malawi style. Choncho katangale angathe ku Malawi. Nkomwenkomwe Chilima sangayime pa president as thye law forbids him.

    • @russellsombwa1609
      @russellsombwa1609 Рік тому +1

      DC Bon kalindo wanena yese akusapota mbava mchitsiru

  • @moses372
    @moses372 Рік тому +4

    Chilima ndi machine

    • @stevemkanda-zz4gr
      @stevemkanda-zz4gr Рік тому

      Aaaaaa zokuba basi anthu mene akuvutikilama kumalawi eya

  • @msaiwaleumandi6077
    @msaiwaleumandi6077 Рік тому +4

    Afuna kumunamiza Chilima anthu

  • @manasemaposa
    @manasemaposa 3 місяці тому

    Bhazuka machine Dr SKC

  • @msaiwaleumandi6077
    @msaiwaleumandi6077 Рік тому +6

    Chilima akachoka ku Mcp , chipani chowina ndi Dpp

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 5 місяців тому +1

    Chilima is not a thief, it was just a move by MCP to turnish his name So that he doesn't stand in 2025. It was well calculated by Chakwera.

  • @sgemshane3645
    @sgemshane3645 Рік тому +3

    Ayise Ngati ukufunya gayiwa bola usikafuna maganyu kuchomerera mbamva amwene😱😱😱😱

  • @RofinoJastenJasten
    @RofinoJastenJasten 2 місяці тому

    Chilima

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 5 місяців тому +1

    Chilima mashine

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Рік тому +2

    Aaaaaaa koma umbuli ndikhani zina,,,kumbera mfiti m'manja

  • @EmercianahKasiku-en6hl
    @EmercianahKasiku-en6hl 6 місяців тому +1

    Tapelekani ma comment mukusowa chonena because the guy muli nzeru osati sewero and titamupanga kukhala president wa dziko lino ndikuuzani munthawi yochepa chabe Malawi atha kusitha tikuyenera kusiya mndale za zipani monga tinachitira muja ndikusakha omwe Ali ndi kuthekera not poti ndi wakwathu ai mkulu analakhula uja wapelekako example Chilima ali bwino ndi Pitala zinthu zimayenda bwino koma atangochoka chipwilikiti mpakana DPP inaluza boma nayoso MCP pomwe inalu ndi ubale wabwino ndi Chilima mesa tinagula fertilizer wa 4.9.99 muno pano bwanji? NDE the guy muli nzeru bad zotukukira dzikoli..abale azanga zoona mukufuna Gogo lotha ntchito LA zaka 82 litilamulire?azikangogona achina Norman Chisale azikaba ndalama, mpakana kutayilita kutisakhira munthu osadziwa chilichose Chimulirenji as vice president abale munthu ukafika zaka zimenezo umapuma orso mwiniwake ananena osakakamiza magogo kukugwilirani ntchito inuyoso munthati kuima ngati president kulibe school ya upresi 6:35 dent lamuro la age limit lija limayeneraso kupanda pass imagine the candidate Ali ndi zaka 80 nde alamulire 2 terms azakhala ndi 90 yrs are we serious ndi dziko lathuli a malawi, mavuto omwe boma iliri ladutsamo agogo aja sakanakwanitsa or pang'ono, Chilima ndi machine akatundu or kuti amene kut apanga press conference mawa ma battery awailesi mumashop amatha malo oonetsa film kudzadza meaning the guy has something special let's try him malawias

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 Рік тому +2

    Wasowa choimba kodi, kodi chimakhala chili chain kumasapota mbavazi

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5o 4 місяці тому

    sitikufuna anthu otibera misonkho yathu onse atonse alliance alibe CHOTI angatiuze ife amalawi zotinamidza ife tatopa Nanu nonse mbava zokha zokha

  • @mustafailanga2585
    @mustafailanga2585 Рік тому +1

    Zachamba chilima mwanva!!!

  • @clementmahoka6287
    @clementmahoka6287 5 місяців тому

    Chilima machine

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du Рік тому +1

    Kuombera fiti manja mbava yeniyeni

  • @user-xe1so5xj2w
    @user-xe1so5xj2w 6 місяців тому

    Chilima ndiwakuba mupaka nyimbo guys

    • @user-le9su3mt7r
      @user-le9su3mt7r 5 місяців тому

      Wakuba mambo wako chakwera na pitala chilima bomaa

  • @danielzitande5231
    @danielzitande5231 9 місяців тому

    Kkkk mmmm koma mudziyimba kuti Chima wakubayeeeeee! Komanso wabodzasaaa, mukadzamuvotela Chilimayeee, adzabayeeee.

  • @abdulrafiquekalembo469
    @abdulrafiquekalembo469 6 місяців тому

    Kujoinana ndi MCP kuja pakokha it was a very big mistake and nkhanza that he did to Malawians.Ndiye poti aMalawi ambirife tinalodzedwa/opepela zinthu ngati zimenezi samaganizira kuti tikuvutika ku Malawi chifukwa cha decision imene iye anapanga yolibwezeretsa boma la nkhanza m'boma.Atleast akanayima payekha Kapena kujoinana ndi chipani China chake olo Aford.Koma MCP!????.Ayi ndithu people uyu mngwaphuma kwambiri uyu ndipo wa dyera musadzayelekeze kuononga vote yanunso pa uyu.God forbid

  • @user-gd7xm7xr9v
    @user-gd7xm7xr9v 6 місяців тому

    Mmmmm
    Mbava

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 5 місяців тому

    Mukufuna apitilize kuononga zakeso et gwape ameneyu angakhulupilire ndan

  • @mathewsmbaluko8522
    @mathewsmbaluko8522 Рік тому +1

    Zopusa mwaponya apanu mukusowa chochita😲

  • @bernaddickson
    @bernaddickson Рік тому +2

    Km zowona zonsezi tikumvadi ukuwawatu ndi ATONSE ALLANCE

  • @abdulrafiquekalembo469
    @abdulrafiquekalembo469 6 місяців тому

    Munthu wa dyera uyu.Anatenga kuwachotsetsa achinyama ku ulamuliro wabwino wa DPP umene zinthu zinali bwino kuwapititsa ku Ng'ona za MCP.Zonsezi anapanga chifukwa cha dyera ndi Phuma ndi upresident.Only anthu akhungu mosaona patali amagomera Chilima

  • @dicksonilimbani3443
    @dicksonilimbani3443 Рік тому +2

    Akuba ngati ameneyi

  • @abdulrafiquekalembo469
    @abdulrafiquekalembo469 6 місяців тому

    Inatimvetsa kale kuwawa ameneyu tilibe naye mau.wabodza, ofowoka.

  • @dingim1234
    @dingim1234 Рік тому +1

    Chilima si mbamva zili ku MCP. The most effective way to destroy people is to deny and obliterate their own understanding of their history. Thats propaganda.

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 4 місяці тому

    Munatinamiza kale inu sima yodya katu ija ilikuti munataya geme
    Nokha basi

  • @abduljafari7387
    @abduljafari7387 Рік тому +1

    Koma ndiye mwalawilila chitukuko tinasachione ko iwe ndi mbuzi ndi thu

  • @yahiyajonse
    @yahiyajonse Рік тому +1

    Koma satana ndi oopsa guys eerr

  • @idris6597
    @idris6597 Рік тому

    Mboli zanu

  • @juniornaphazi4852
    @juniornaphazi4852 9 місяців тому

    Awandiopusa inu

  • @EmercianahKasiku-en6hl
    @EmercianahKasiku-en6hl 7 місяців тому

    Chilima ndi 1 palibeso make pandale mdziko mino

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 6 місяців тому

    Amakumbukira ADAD uyu kuti anali .munthu wabwino... pano manyadxi okha okha ... ADAD ananyodxedwa kutukwanidwa kusemeredwa nyatsi koma ADAD anali pheee kumvesera .lero chilima wangoyetsa kupanga matukutuku mmmmm mcp yati aaaaa mwanayu sakuidziwa mcp ndiyesa anali mwana 1987 koma timuonese anaona Muwaro ndi Gwede .lero uyo

  • @user-wd7lk7nx7m
    @user-wd7lk7nx7m 11 місяців тому

    Koma misala ina iyi

  • @mussahcassim4963
    @mussahcassim4963 Рік тому +1

    Zaziiiiii

  • @mandamandamanda2208
    @mandamandamanda2208 Рік тому +2

    Amene ukuyimba nyimbo yako yopusa naweso ulimugulu lambava zoopsya m.malawi muno muhanya uno munthu wanzeru zake angavotereso chilima mbava ya zuneth satar iweso ndiwe garu umanamiza dziko kuti anthu adzadya katatu azagura fertilizer 50kgs pa mtengo wa k4950 zikutheka Lero chilima ndiye munthu woyipa kwambiri 50kgs fertilizer mpaka na k90. 000 stupid foseki akagwere uko

  • @usumanimusa411
    @usumanimusa411 2 місяці тому

    Kuchenjres akulu awa apit nazooo kumanda