Розмір відео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показувати елементи керування програвачем
Автоматичне відтворення
Автоповтор
Prodigal sons and daughters are busy disliking these beautiful songs.
Ife ndife amalawi good songs mphungungu Joseph kasa
Kuimba ndikuitanidwa kwanu ankasa, nyimbo zanu zabwino kwambili. Muzitipatsabe nyimbo zina coz Malawians we proud of you and nyimbo zanu zimatipatsa chilimbikitso tikazitsatsa, tiyamike mulungu ndithu
This is a hot song of patriotism.......IFE NDIFE A MALAWI
U just know... Ndife Malawi
Nkasa umatokosa palipose kuti tiyende mowongoka, malangizo abwino mulungu apitilize ku kusamalani ndi banja lanu !!!
munthu wankulu Yahweh akudalitseni Che Nkasa
I like this man he's gifted & has wisdom when listening to his songs are full of advice that bring us into one trail, nkasa long live long live !!!!
Cop Nyasulu
3wwwďs32àâ
okonda kunamizidwa ziveleni nokha.Okonda kunamiza azanu nanunso dziveleni nokha.langizo labwino kuchokela kwa nkasa.
kkkkk komadi iyiyi-iyi yomakupatsa ulemu ukafayidi ndichipongwedi chachikulu ......IFE NDI FE A MA LA WI
Nkasa ndinu phungu!
Ife NDI Ife amarawi km iwe ulid ndi luso ndipo uzithokoza mulungu
Akulu a NCHITO bambo Joseph nkasa.
Phungu j
mwandikumbutsa kale nkasa amatha
Mkasa ndi katundu amwene eee
mumakwana abwana more fire koma musamayimbe za ndale
Ndine Bikitoni Nsandamila Akadzasiya obena Nkasa adzasiya Ndare
Kkkkkkkkk ndi kuva
Mphongo iyiyi ili ndi mayitanidwe
Mathews makina zilibwino chenkasa
Mkasa amaimba
good
Phungu Joseph Nkasa,Millionaire
Fatastic
Prodigal sons and daughters are busy disliking these beautiful songs.
Ife ndife amalawi good songs mphungungu Joseph kasa
Kuimba ndikuitanidwa kwanu ankasa, nyimbo zanu zabwino kwambili. Muzitipatsabe nyimbo zina coz Malawians we proud of you and nyimbo zanu zimatipatsa chilimbikitso tikazitsatsa, tiyamike mulungu ndithu
This is a hot song of patriotism.......IFE NDIFE A MALAWI
U just know... Ndife Malawi
Nkasa umatokosa palipose kuti tiyende mowongoka, malangizo abwino mulungu apitilize ku kusamalani ndi banja lanu !!!
munthu wankulu Yahweh akudalitseni Che Nkasa
I like this man he's gifted & has wisdom when listening to his songs are full of advice that bring us into one trail, nkasa long live long live !!!!
Cop Nyasulu
3wwwďs32àâ
okonda kunamizidwa ziveleni nokha.Okonda kunamiza azanu nanunso dziveleni nokha.langizo labwino kuchokela kwa nkasa.
kkkkk komadi iyiyi-iyi yomakupatsa ulemu ukafayidi ndichipongwedi chachikulu ......IFE NDI FE A MA LA WI
Nkasa ndinu phungu!
Ife NDI Ife amarawi km iwe ulid ndi luso ndipo uzithokoza mulungu
Akulu a NCHITO bambo Joseph nkasa.
Phungu j
mwandikumbutsa kale nkasa amatha
Mkasa ndi katundu amwene eee
mumakwana abwana more fire koma musamayimbe za ndale
Ndine Bikitoni Nsandamila Akadzasiya obena Nkasa adzasiya Ndare
Kkkkkkkkk ndi kuva
Mphongo iyiyi ili ndi mayitanidwe
Mathews makina zilibwino chenkasa
Mkasa amaimba
good
Phungu Joseph Nkasa,Millionaire
Fatastic