Abusa akanika kuvomeleza kuti ishimaili ndi mwana weni weni wa Abraham abusa akukana Pati akanakhala kuti Mwana okaikitsa Mulungu sakanapelekako utumiki mbali yakumtundu wake abusa mwatani kodi
Mwana wa lonjezo ndi Issac not Ishmael Ndichifukwa Mulungu sanatsutsana ndikuthamangitsidwa Kwa hagala chifukwa hagala sanali mkazi waubwana wa Abraham
Abusa kulongorora ndikumene akuziwa nanga zomwezi pakhatukhuta😂😂😂😂😂
Ndine osangalala kukhala mcristo 😂😂😂😂😂 amen.
Amen mustafa
Ndineosangarala kukhala musilimuu
Ambuye 😂😂😂😂😂 ndakondwa zedi yesu ndi fumudi yo chokera kwa ino.
😂😂😂abusa kubisala mbatata ssana panja😂😂😂😂😂🤕
Kodi pankhani yoti anapelekedwa nsembe ndi Isake kapena Ishmael muliphindu lanji kwa ife anthu?
Funso limeneli atsogoleri athuwo sadatiyankhile
Chirungamosungabise abuzza kkkkkkkkkkkkk samanyazi
ABUSA makani ngati mwatumidwa ndi SATANA.
Mmmmm koma Abraham mumalakwira chifukwa sanali osutsana ndi mulungu
Where’s part 2. Congratulations Bishop for proving Islam wrong. RIP
Abusa aboza amenewo mulungu awakang'anthe manda mene alimo pamozi ndiowasatila onse amene ali moyo ndikutanthawuza kuti akhristu nonse
From originally mwana woyamba ndi isake chifulkwa Ismail adabwadwira kwamkazi wantchito
simudziwa kanthu akulu inu,,,kd mwana oyamba wa Abraham ndindan🤣🤣🤣🤣
Ishumael ndioyamba coz abrahmu anakagona ndi mzakazi cz sara anamakanika kubala.
Koma asilamu paboza alibe manyazi
Kkkkkkkk proudly Christian
Abraham sanapemphe ismaeli ayi,pempho la Abraham linali kwankazi wake sara
Ntukula unali big....rest in internal peace.....
Pali chimene anayakha pamenepo mukuti ntukula wanuo mmmmm
km abusa awawa akudziwa kut baibulo silinasiidwe nd yesu mwini wake iziz akulankhula apa zachina poul ndazizake
Chi islam ndi kusochela 😂😂😂😂ndi onamaso anthu ake zigololoso thopo mpaka ndawi yofunga mukalangidwa.
Abusa a mtukula Rip mumatha kulalikila mawu a mulungu
Pamenepo analalikila akukanika kuyakhawo kod inu mumakacheza ku church ⛪kujatu et
Amustafa mukuchulusa bozatu apa
Malibe Zina la Ishmael mu verse imeneyi...Dayilesi akunama........
Koma kuchisilam kuli nkhungu losayamba,
Abusa akanika kuvomeleza kuti ishimaili ndi mwana weni weni wa Abraham abusa akukana Pati akanakhala kuti Mwana okaikitsa Mulungu sakanapelekako utumiki mbali yakumtundu wake abusa mwatani kodi
Khani yakuku ndi Zina lanu?
Mwana wa lonjezo ndi Issac not Ishmael
Ndichifukwa Mulungu sanatsutsana ndikuthamangitsidwa Kwa hagala chifukwa hagala sanali mkazi waubwana wa Abraham
Ismail odetsedwa tigayile lemba
abusawo sakuziwa chimene kurani ikunena
Inu mulungu mum udziwe musanizidwe mulungu anadalitsa sarah ndi mbuye yake
Without doubt Islam is false.....