CRUISE 5 WITH PETER DIMBA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лют 2025
  • ZODIAK TV NEWS

КОМЕНТАРІ • 81

  • @elubymkusankhoma330
    @elubymkusankhoma330 8 днів тому +13

    He avoided certain questions, but from the ones he answered, he comes across as quite honest-a rare quality in politics.

  • @henryngwira8188
    @henryngwira8188 6 днів тому +5

    Joab you are a good journalist,umafunsa mafunso mosapanga attack munthu komanso mafunso okhwima,osati ena omwe timawaziwawa,omwe amapanga za personal pomufunsa munthu ndikumupanga attack,namangobwelezabweleza mafunso

  • @alexmajanja3179
    @alexmajanja3179 3 дні тому +1

    Amene muti sadziwa chomwe akunena or ndi mbuzi. Munangozorowela kut ma poticians adzikunamizani. What an honest guy he is. We need more leaders like him .... Leaders who can admit pomwe zinthu sizikuyenda bwino

  • @PempheroLyson-f2s
    @PempheroLyson-f2s 3 дні тому +1

    Peter Dimba inspires me alot❤ remain blessed boss

  • @ChifundoKapesa
    @ChifundoKapesa 6 днів тому +1

    Joan!!! You are a genius...... Peter Dimba too is one

  • @tgf2240
    @tgf2240 7 днів тому +5

    First time seeing a politician who is not political. Composed, humble, honest, remorseful and brilliant. Explaining things like an ordinary person without being pompous. Big up Hon Dimba

  • @jacdimbadimba1679
    @jacdimbadimba1679 8 днів тому

    Hon. P Dimba, you always impressing my heart. Keep it up!! MVULA kumudziko akuti ikubwera bwino- Rev. J Dimba.

  • @KamnedyKambani
    @KamnedyKambani 4 дні тому

    Big up to hon Dimba ,he's humble and honest , and when the government arrested opposition politician who concerned with corruption ,the same malawian came to say it's political issue if is not true anthu opusa ife

  • @Harrisonchiswara
    @Harrisonchiswara 2 дні тому

    Kmaso Joab mwavala bwino 🔥🔥

  • @GrantMombera
    @GrantMombera 7 днів тому +1

    Salute Mr Dimba for your Honesty. I hope this is really u

  • @CharlesAmosiKapalamula
    @CharlesAmosiKapalamula 8 днів тому

    This is guys is very good. I have honestly liked you. Very honest and intelligent MP

  • @KelvinMandelaChirwa
    @KelvinMandelaChirwa 3 дні тому

    I salute this man , humble

  • @AtusayeNyirenda-b5x
    @AtusayeNyirenda-b5x 5 днів тому

    Joab Busy making History, big up bro!!

  • @evelynmzonde4432
    @evelynmzonde4432 3 дні тому

    We need to have more honourable like this,I salute you bwana

  • @DadTshepo
    @DadTshepo 6 днів тому +1

    This Guy is Good n Honest kma Ali mbali yolakwika mwaiye kachilungamo kalimo kma wazungulilidwa ndi ng'ona I feel sorry for him

  • @dumisanindhlovu6415
    @dumisanindhlovu6415 8 днів тому

    Hon Peter Dimba ndi Katswiri !, a very rare kind, I like this guy !👏👍

  • @felixellard7555
    @felixellard7555 День тому

    Joab ndi dolo
    Fadawa ma crucial questions angowapondatu🤣🤣🤣

  • @sunganikaphamtengo9280
    @sunganikaphamtengo9280 4 дні тому

    One honest Politician in Hon. Dimba

  • @BrightonNdalama-x2b
    @BrightonNdalama-x2b 5 днів тому

    Hon deputy minister u seem honest though you're deliberately failing to tackle certain crucial questions and it shows that you're hiding or you're protecting ur government that's what I have discovered from this interview but we'll done Mr j chankhaza

  • @LovemorePeeches
    @LovemorePeeches 4 дні тому

    Honorable l use to know you through kindness, humbleness

  • @BilliatEvance-kr1mh
    @BilliatEvance-kr1mh 6 днів тому +1

    We need to do more in our politics. Our politics from since the so called independence is a scam we need to take the path of Denis Mahata.

  • @charleskunjawa6999
    @charleskunjawa6999 4 дні тому

    Koma Dimba, you remember your lecturers well well... Nthindwa, mwamuna wake wa Ruth wa UCCC kkk

  • @JuniorSaine-d6r
    @JuniorSaine-d6r 8 днів тому +1

    I think your the guy 🔥..but am finding some difficulties on water transportation,I don't think government can manage to operate such transportation.palibe chomwe chuyenda with government.

  • @JamesIdrissahHussein
    @JamesIdrissahHussein 7 днів тому +1

    Koma 😂😂😂 Joab Unabadwa Thawi yakamuzu mot ndiye siukulat ngati Lulu 😅❤

  • @jamestewesa1046
    @jamestewesa1046 7 днів тому

    Zimangofunika leader azikhala ndi experience. Angakhala minister of finance awa..? Nice nice kma.

  • @giftjahkaykatunga9417
    @giftjahkaykatunga9417 7 днів тому

    joab ur the best interviewer in malawi i watch alot of interviews but how u ask its comfortable for someone to answer even if he/she doesnt want to answer

  • @HappyBorderCollie-od3le
    @HappyBorderCollie-od3le 8 днів тому +2

    U have mu vote as my area Mp but on party eeesh prove me well on economy.how can we buying 3700 dollar

  • @hassanabdullah9184
    @hassanabdullah9184 4 дні тому

    Aaah aaaa ma guy😂

  • @ChikuByson
    @ChikuByson 7 днів тому

    The honourable seems to be an honest and intelligent i like that about him

  • @FrankNedson
    @FrankNedson 8 днів тому +2

    Mbuzi ya munthu iyi amangofuna vote Koma kuthandiza anthu ake ai mnabetsa vote yanga .....Zaka zambiri mbiri koma kulephera kuika Phula nseu kwao, zipatala,madzi aukhondo 😭😭

  • @NikolasNanawe
    @NikolasNanawe 8 днів тому +1

    Dimba🔥🔥🔥👑

  • @georgedesiremkamanga2210
    @georgedesiremkamanga2210 8 днів тому +2

    Big up bwana Dimba, muli kachilungamo mwa inuuu!

  • @charleskunjawa6999
    @charleskunjawa6999 4 дні тому

    Paja nthawi imeneyi ntchito accountacy department imachita kutifunsira ... kkk

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 5 днів тому

    Ngati ku MCP kuli anthu abwino 5 Mr Dimba muli mommo

  • @EmmasBwe
    @EmmasBwe 7 днів тому +1

    Uyuyu saziwa zomwe akunena

  • @jamespagona8140
    @jamespagona8140 4 дні тому

    Ma biggie munapezanatu macheza abwino awa

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 2 дні тому

    Interview iyiyi ili bwino ndi Nduna iyi umunthu ukumutsutsa koma mbali yake yaikulu akudziwa kuti MCP siili bwino.
    Imagine za Chizuma President anakana kuti sanadziwe yemwe anatuma a polisi kukammanga.Panopa MCP ndiyolemera kuposa mmene inaliri 2019 pomwe imadya ndalama za Mia.
    MCP ndalama yazitenga kuti?

  • @AnthonyMaluwa-l4k
    @AnthonyMaluwa-l4k 8 днів тому +2

    Akakhala pa nkhate.

  • @TheCurios-Mind
    @TheCurios-Mind 8 днів тому +2

    Ameneyu ndi mbudzi bwanji.

  • @charleskunjawa6999
    @charleskunjawa6999 4 дні тому

    Kikiikiki Thengolose --- ati Then go lose amazuza anthu uyu. kaya ali kuti mkulu ameneyu

  • @GrantMombera
    @GrantMombera 7 днів тому

    Dimba you are amazing

  • @DavieGoodson-s5t
    @DavieGoodson-s5t 7 днів тому

    Joabu wagonjesa nduna ndimafunso, nduna ikukanika kuyakha mafuntso ingozikola
    Ikuteteza mpando wake padakalipano sangayakhe chilungamo

  • @jamestewesa1046
    @jamestewesa1046 7 днів тому

    2000 14 points za nice..

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 6 днів тому +1

    Joabu umakwana

  • @charleskunjawa6999
    @charleskunjawa6999 4 дні тому

    a classmate anthu, a poly UCC cong rep. mumatiimilira inuyo

  • @Mikelemiphert
    @Mikelemiphert 6 днів тому

    Bodza, Malawians don't highly regard MCP, it's undemocratic, and u shld provide ur evidence in the court of law that DPP murdered Njaunje, this is a serious allegation and u must prove it. Anyone found guilty shld face the law, why keeping silent?

  • @blessingsgatoma2607
    @blessingsgatoma2607 4 дні тому

    Dimba ndi dolo

  • @duncantonnykapunda7639
    @duncantonnykapunda7639 8 днів тому +1

    Zinangowona kuchitika uyu kukhala wa mcp, koma alindinzeru kupotsa chakwera.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 7 днів тому

    Mwati awawa ndi deputy minister? Mnyamata wabwino bwino koma zero pa 10.

  • @PatrickMaster-m3i
    @PatrickMaster-m3i 7 днів тому

    Achakhaza apa mukucheza ndi bulutu weniweni akuyankha zosemphana ndizomwe mukufunsa

  • @darlingtondlipenga8145
    @darlingtondlipenga8145 6 днів тому

    MQT😂 eeeh achina Simulation

  • @ChimazileJoseph
    @ChimazileJoseph 7 днів тому

    License mungopeleka zipepala ku road traffic

  • @JamesYassin-n7t
    @JamesYassin-n7t 8 днів тому

    But jowabu chakaza umakwana ndipo umafunsadi mafuso abho ndipo adimba akulephela kuyakha komaso tiwayamikile Zina akuvomeleza

  • @idrissahyunus-fp2yv
    @idrissahyunus-fp2yv 7 днів тому

    Mchifukwa chake Malawi wathu yu sakuyenda bwino munthu wa za Ulimi sangayendetse unduna wa za Maphunziro kumeneko ndy kulakwitsa zinthu

  • @alfredmmora3676
    @alfredmmora3676 8 днів тому

    Joab umabebetsa iweyo

  • @JamesIdrissahHussein
    @JamesIdrissahHussein 8 днів тому

    Munthu wamoyoo angamapange za MCP koma?

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 5 днів тому

    Ka Mr Smile Dimba

  • @AmanaKaisi-p3e
    @AmanaKaisi-p3e 8 днів тому

    Muzijambulila panja za showing off

  • @NoelKhwimba-bh3ts
    @NoelKhwimba-bh3ts 7 днів тому

    Anzangawa amakonda kuseka😊😅

  • @chubwi-k3s
    @chubwi-k3s 7 днів тому

    Phwete basi

  • @GiftZuze-ge1ne
    @GiftZuze-ge1ne 8 днів тому

    Aise iweyo umakwana wandisangarasa usamusiye zaka 5 ndizamber azao amakhra 4 km kukoza zithu

  • @DavieGoodson-s5t
    @DavieGoodson-s5t 7 днів тому

    Joabu wagonjesa nduna ndimafunso, nduna ikukanika kuyakha mafuntso ingozikola
    Ikuteteza mpando wake padakalipano sangayakhe chilungamo