Koma ndalama zonsezo mwatchula Mr kawale ife osauka sizikutipezabetu tili mbuu mmidzi muno akutidyera ndalama zathu ndi ndani? And this is October kuli AIP sikukudziwika. Kummwera kuno tangotsala ndi 2 to 3 weeks kt mvula igwe. Manyazi bwanji kunamiza dziko.
Anthu opusa awa anenazi zosanveka wht not take that money kupititsa kokagura fertilizer then nkumutsitsa with 50% kuti aliyese athe kufikira than ngongole zoti sionse omwe angapatsidwe
Kodi mwati awawa ndi nduna ya ulimi kapena wankulu wa neef??akanangofotokoza za ulimi ifetu zoti anthu akulandira ngongole sitikudzidziwa nde tikuchosa Chanel yi mwina tingonverako nyimbo
Km group ya anthu kubwereka 1,000,000 nde ndchimodzimodzi nd matumba awiri a AIP😅😅😅😅
Ingomvomelezani kt mwalephela kugaila anthu fertilizer musati mango masamba zija ndizowona zomwe anthu alankhulala zija kt muli be fertilizer zija ndinu zisilu bwanji kd mukumatitenga ngat ife ndi anthu ogona kt muzingotinamiza et mbamvaaa
nb
Pni /;blxAs😊w😃🥰😅😁🥰n😊
Alomwe agundika kutukwana
Nde pakusiyana pati pa mathumba awiri out of 200 thausand ndiwe garu kwabasi ukuona ngt anthu alibe masamu
❤❤ KAPE AMENEYU MUSIYENI
Nzeru zanuzo a minister ndi zopoila coz ,1 million devide by 5 it's = 2 bags of fertiliser per person. Of which is expensive than AIP.
Koma ndalama zonsezo mwatchula Mr kawale ife osauka sizikutipezabetu tili mbuu mmidzi muno akutidyera ndalama zathu ndi ndani? And this is October kuli AIP sikukudziwika. Kummwera kuno tangotsala ndi 2 to 3 weeks kt mvula igwe. Manyazi bwanji kunamiza dziko.
You must do action kuti zikupeze ,, kuteloko chakachino anthu ena azipexa
Kod ndiazizake ndiaja anagula fertilizer ku butchery aja??
Nice articulation, Minister.
Mbamva inu kwanu kwatha basi muchoke tione zina mukungoyankhura mfundo zopepera basi ndalama zamisonkho yanthu mukungoba basi amphawi kumawanamiza . Achakwerawo aiwala zomwe ankatilonjeza zija eti.
Just want to know if these are loans or grants to Malawi?
Ambuye tithandizeni wakumuzi uja wafa ndinjala bas
Well said Mr minister, however my question, do we have the market
A Minster Kawale, mukuti forex yikusowa nanga zoyendela maulendo zimapezeka kuti
Anthu 5 agwirizane kukatenga 1 million, , meaning 200 tau per person, amenewo si matumba awiri?
Ndale zanuzi nzaboza a MCP and neef.
Brian ukumvesera zopusazo ziitana anthu amene azikamba zothandiza Zimene akukambazo ife sitikuziwona
Ndinu ambuli ndeti
Agricultural sector has registered tremendous positive impacts yet the country is still languishing and starving are you sure Mr Minister?
Ndie mukuibwereza dala malo amodzi modzi video. Timadziwa kuti mumafuna kumuipisa munthu. Koma amalawi ozindikila pano sadalila AIP chifukwa or anthu alandile zimenezi amatha mkugulisa. So kwa ife amane focus yathu ili ku ulimi. Timadalilaso manure aziweto zomwe tili nazo.mpaka timakolola phwamwamwa chosecho AIP sinatikhudze.
Boma ndilomweli tikupasan mpata mu 2045.
Soka kwaine sinapiteko ku sukulu kamba kaumbwawi kom ngat mister of agriculture sakiganiza zongotsitsa mtengo wa feteleza kut mulimi azitha kugula bobho alibbusy kumangokamba zandalama ife tilibe😅
Uyu ndi galu kwambasi
Nduna yakuba iyi palibenso chomwe akunena apa nzautsiru basi
Kuti dzisiru kokatenga ndalamadzo instead Kuti inu mukagulire fertilizer kapena kukapereka kumakapani a fertilizer Kuti asike
62 billion
70 billion
Ndiye Kuti chani😢
Aaaaaaa umati Anthu asabereke mukungodya ndalama agalu inu
From the interview zaonetsa kuti fertiliser kulibe plus mavuto Ku AIP ngochulukaso
Anthu opusa awa anenazi zosanveka wht not take that money kupititsa kokagura fertilizer then nkumutsitsa with 50% kuti aliyese athe kufikira than ngongole zoti sionse omwe angapatsidwe
Koma minister uyu mabatile ake akuyankhula ngatii position iyi wayitenga zulo
Anthu ali busy kutukwana azawo akutenga ndalama kumapangira business
Ngati pali unduna umene kuli bodza lochuluka komaso umbava ndi umeneu ndipo nduna imene ndi imene yabweletsa njala ku malawi
😂😂😂😂 Mr tell us how many people did get that money chomwe chilipo ndikudya ziteze bassss
Mmmm kukometsa pa kamwa abale. Nthawi ndi ka mnyamata. Zioneka.
Fotsek! 4500 amanena uja ndameneyu
Mwakanika kukwanitsa kukhala ndi chakudya in four years do you think u can manage in less than a year 😢😢???
Alp is Alp don't change where to get those money
Wakuba uyo ndi chakwela wakeyo
Kd akati munthu azikhala ndi fetereza okwanira akutanthauza chani
Akuti fertilizer uja matumba awiri mutha kuwapanga kukhala ten ndiekuti mulima malo ochuluka
Kkkkkkkk am confused @DeveliousMasinja
Mpumarang
vuto bomali ndilosamva zomwe amalawi eni akufuna tinati zopereka zaulelezo zisiike tangotengani ndalamayo mukapereke kwa Admarc anthu azigula motchipha basi njala yatha
Awa apapa akuonjezela njala osat kuthesa mbuz athu imoz ithandiza chani. iii tafa basi
Patumbo pamako phwokophwoko pamaphwisipo
Iiiiiiii dziko lathu boma ili ayi or mukati boma lomwero za manyazi kwambiri
Ndiwe galu kwabasi
From AIP to Katapira . Neef izakulanda nyumba kkkkk
Ukalephera kubweza eya
Greedy ndiyomwe ikupangisa malawi azikhala ndi njala anthu oyipa inu
Agalulu inu opanda chifundo
Zakumbolo basi
Mufuna kuchosa subseed thus points
Anthu oipa
Zaulelezi zimatipha nzeru
Bodza likuchita kutuluka kamwa malo mwa million mukuti thousands ai xikm 😅😅😂 tinamizeni km mau anuwa tawasunga
Chitsiru iwe mbamva yachabe chabe ulibe choyankhula galu iwe
Eeeee munayambana naye chani a bwana, ngati muli awuletsi olo at akukupatsani zawurere dzaka teni simungapindure
Iwe utilakwisa
Kodi mwati awawa ndi nduna ya ulimi kapena wankulu wa neef??akanangofotokoza za ulimi ifetu zoti anthu akulandira ngongole sitikudzidziwa nde tikuchosa Chanel yi mwina tingonverako nyimbo
Zachamba
Koma mbudzi idzi you have still talking about covid koma kungoti mumabera alimi afodya pobwedza ngongole dzanuzo
A bag of money it won't heal poverty on your statement you only talk about money money teach people to discover them self.
Palibe company ya kunja ingalole ma kwacha zimenezo ndizaboza
Kuti dzisiru kokatenga ndalamadzo instead Kuti inu mukagulire fertilizer kapena kukapereka kumakapani a fertilizer Kuti asike
62 billion
70 billion
Ndiye Kuti chani😢