Uwu akuyankhula mwauchisiru ndale zokhazokha he's not speaking as a minister of Malawi but as MCP minister and that's foolish.Panopa things are worse kaya
Amalawi sadikira wina kuwawuza zochita lero, maso athu siakhungu chilichonse tikuwona and tikudziwa, kodi mudapha ku chikangawa tikuwona aja plus witika tikudziwa, agalu anthu oyipa.
Ine ndingofusa nao kod mfumu angaweluze mulandu was mwana wake kapena amfumuo kuweluza mulandu was chemwali ao chikuvuta chani ngat palibe vuto kwachosa anthuo chikuvuta chani kwa achosa mmayesa muli okhozeka ikaniponi Ena mutamangisane pa ground
Chakwela mushona ndi buzi, So president Chakwela ndi phwala mu zonse. Let's exercise our democracy speak ur mind sangakunjateni mutukwaneni president chakwela kuti Pantumbo pake enjoy ur democracy. Ndatha ine Ben Longwe chikuni chautsi delela nyani
Kupatula za ndale ineyo Moses Kunkuyu amandiyankhulira mwa mzeru kwambri❤❤❤❤❤
Zelu zake ziti nenani
I think atola nkhani ali pamenepa nd a mcp
Za commission of inquiry ya ndege komanso zachi machine ku MEC simukuyankhulapo bwanji? Mxiiiew!!
Uwu akuyankhula mwauchisiru ndale zokhazokha he's not speaking as a minister of Malawi but as MCP minister and that's foolish.Panopa things are worse kaya
Plane crash inquiry bwanji sakufotokoza 😂😂😂😂
Chikangawa aaaaaaa aiiiiiiiii Bingu si inuyo mupha 123 kupatikiza chilima
Kodi nkhani ya wittika ija mukuti nayo bwanji poti akunkuyu munamupha chifukwa cha hule 😢😢😢😢
Hahaha nde zikukanika bwanji kuli fotokozera dziko kugwa kwa ndege ija ku chikangawa komaso kuti a president anatinamiza
Palibe fundo apa uyu ndikapetu ndipo dpp my vote
aaaaaa palibe chamzelu apa zachimachini sakuyankhapo zandege sakuyankhapo kuthamangila zaziiiii
Koma mafunso ake ndiye odzidzira, atolankhani ake amenewa bwanji
Musamanamizile amalawi ayi kod mukuti Madina akubwelerao kwa one ndili kumudzi pindu ndi chani panopa
Makhulupila kukambilana lelo akukuyu inalipo nthawi yomwe sauli ama ntchingila njila Davide kupangila chiwembu chosiyana siyana koma mapeto wake Davide anakhala mfumu
Where is commissional of inquiry
Pangani fundo fundoless galuwe amene utm inachoka manganya si president wa utm aiiiiiiiii choka
Amalawi sadikira wina kuwawuza zochita lero, maso athu siakhungu chilichonse tikuwona and tikudziwa, kodi mudapha ku chikangawa tikuwona aja plus witika tikudziwa, agalu anthu oyipa.
Ine ndingofusa nao kod mfumu angaweluze mulandu was mwana wake kapena amfumuo kuweluza mulandu was chemwali ao chikuvuta chani ngat palibe vuto kwachosa anthuo chikuvuta chani kwa achosa mmayesa muli okhozeka ikaniponi Ena mutamangisane pa ground
Bwanji mwalankhura zomveka zomwe ineso ndimafuna kuriuza dziko la Malawi 🎉
Chakwela mushona ndi buzi,
So president Chakwela ndi phwala mu zonse.
Let's exercise our democracy speak ur mind sangakunjateni mutukwaneni president chakwela kuti Pantumbo pake enjoy ur democracy. Ndatha ine Ben Longwe chikuni chautsi delela nyani
Iwe paja ulisotu ndimulandu wakupha pano sukuzengedwa chifukwa uli muboma tikumana 2025
Sizimenezo akunku tikuti ife tilibe ma I'd tikavote inuyo muchoke bomali sitikulivuna chitukuko chake chiti zautsiru basi anthu akupha inu
Bwanji osawasiya a mec kuti aziyankhile okha? Kusiyana ndi uyu m'neneli wa boma yu
Mesa sipika wan uja samalongosoka,,,koma guys ngat mudalila ndalama mwabazo ndithu muzuzisa makolo anu
Anapha phwitika ndi ndan ? Koma akulu ngat mukulitenga ngat zikoli ndi lamaja mwan, ayi wina achimina
Boma la mcp linalowa ndi mademo inu mukukaniza mademo pali zelu
Amalawi tikudzindikila sopano olo inuyo zonse mukulakulazo siza amalawi ayi ndi zanu kod kulolelana kuli kuti ngati mumapanga zithu zanu pambalambanda aloleni amzanu zomwe akufuna na ngatidi palibe cholinga mmayesa zithu zanu za pambalambanda
Onama ndiwe. Tikuona zalero
machende ako konkuyu unapha alani witika
Khan ya witika ilipat
Aaaa machende wakho iwe konkuyu ndigulu lako
WITIKA ARI KUTI MCP YATIKWANA KUKUYU KOMA INUYO CHILIMA ORDER FROM ABOVE TO KILL 8 PEOPLE
Mwambiwo nde mwatinamiza vuto munamupha mwachangu nzanu uja mukanaphunzira miyambi. Komaso inu bwanji mukulandila anthu omwe amatukwana MCP yo, fundo zakuthelani
Boma lanu ndi loipa silisatira malamulo
Nanga mulandu wanu bwanji
Chete kulipakula bodza ngat z nzn 😂
Atola nkhani opusa inu osafusa mafuso anzeru
Boma nilomweli zoonadi.osusa anjenjemela
Mbuz yamunthu iwe kwanu ndkupha ndkuba mxim
Dpp musaiware anapha apwitika paja munaiwalaso beana
Waziziwa relo zot madem ndi achabe? 2020 iwe ndizako chakwera sunayende paseu? Mmm ukunama siife Ana uziwaso
Nonse ndi zitsiru nanu atolankhani Mesa mmene mujanso munali nkhani ya enquiry bwanj simunakambeponso mxwee
Iwe moses nkuyu manyi ako palibe chomwe unganene apa inu ofunika kuzamangidwa inu mwazuza mizimu ya amalawi osalakwa mbolo yanu
Kwanu kwatha man
Ankukuyu inu lero mukuona chitsotso chili mmasso mwazanu mwayiwala kuti zanu zitsoso zili mbweee mmaso mwanu mwayiwala boma lanu kuti nslo nachululka zolakwika kwambiri ndibola dpp koma inu fundo mulibe dikirani mutuluke mmenemo ndipamene midzaone kuwawa dziko
awa akuona ngati ndi amuyaya akunkuyu chimwendo chothyola zikhale ng'oma koma afunse kamuzu ali kuti nawonso kuzati ziiiiii 1day
Osafusako za equary yachilima
Unapha witika iwe
Utm sili mu mgwilizano ndi usi yekhayo basi
Moto sufuka popanda moto tiziona marume tazisiyani paja kulikose mumarowa mukufuna kuononga MCp mukamariza kuononga muthawira kt akukuyu
Mmm anthu apha albino why mkulephera kuwamanga, mcp anali kupanga zimene zija kuyipitsa mbiri ya azawo
Nkhope zakuba izi kkkk
Iwe ukutani
Chokupha ichi
Mose
❤
Mcp