BON KALINDO LERO PA 11 JULY 2024 |

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 7 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 117

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 2 місяці тому +15

    Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.

  • @BlessingsMbawa
    @BlessingsMbawa 2 місяці тому

    Bon kalindo iweyo umatha kulankhula bwino. Chifukwa kulankhula kwako umanena zoona zokhazokha kumvera chisoni amalawi munyengo zowawa zomwe tikudusamo kamba ka utsogoleri olephera wa chakwera. Osafooka , osatopa mpakana satana ameneyi tithana naye 2025 ino. Keep it up wakulu ndimakunyadirani kwambiri

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 2 місяці тому +4

    The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅

  • @ThompsonMakwakwa
    @ThompsonMakwakwa 2 місяці тому +2

    Aaaaaaaaaaaaaa@ koma nde zafikapotu mpaka muchenga machende awo ndithu

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah 2 місяці тому

    Bon kalindo dddccccc❤

  • @JibuzahDrag
    @JibuzahDrag 2 місяці тому +1

    Fire Mr president mumayakhula zilungamo zokha zokha

  • @ZephMbeleswa-n8m
    @ZephMbeleswa-n8m 2 місяці тому +1

    Ife si osauka ndipo sitisilira kukhala ndi president osauka😂😂😂😂😂

  • @AbdulsEdsan
    @AbdulsEdsan 2 місяці тому +1

    Mr Kalindo great soldier

  • @AfricanKingdom-uv1qb
    @AfricanKingdom-uv1qb 2 місяці тому +1

    God protect mr DC

  • @ishmaelcassim806
    @ishmaelcassim806 2 місяці тому +1

    Mr bon kalindo you are number one. More fire Mr dc❤

  • @ChrissySalimu
    @ChrissySalimu 2 місяці тому +1

    Sikusinja imweyo kkkkkk taimbaso Mr DC aifeeee❤❤❤

  • @hajrazuwaja4993
    @hajrazuwaja4993 2 місяці тому +1

    😂😂😂amangidwaso uyu ndithu sikusinja ndi gwenembe koma Mr the DC kkkkkkkk

  • @ChristinaSinoyakapawo
    @ChristinaSinoyakapawo 2 місяці тому +1

    Ndabwereza kawili nyimbo yoooo anaphaa mubale wake gwenembe chifwukwa cha udido

  • @Moses51
    @Moses51 2 місяці тому +1

    The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉🎉

  • @julietmussa5103
    @julietmussa5103 2 місяці тому +1

    Sikusinja ndi Gwenembe yemweyo....ana amphunzile

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd 2 місяці тому +1

    Mwana wowopya kwambiri!!!!!!!!!❤❤❤❤❤❤

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje 2 місяці тому +1

    We love you the DC

  • @chrisneySwanepoel-yu5vd
    @chrisneySwanepoel-yu5vd 2 місяці тому +2

    God protect mr kalindo

  • @user-cg5ml7ym4v
    @user-cg5ml7ym4v 2 місяці тому +2

    Tili pa mbuyo panu DC ❤❤

  • @Qspy-b9m
    @Qspy-b9m 2 місяці тому +1

    Powerful Mr president ❤

  • @JosephPindani
    @JosephPindani 2 місяці тому +1

    Km chakwela watopa m'chenga mpaka nd wa boma kkkkkk😅😅😅😅😅

  • @AubreyBamus
    @AubreyBamus 2 місяці тому

    My vote bn

  • @FelistasNkasalaMakumbo
    @FelistasNkasalaMakumbo 2 місяці тому +1

    Ndakhalira kuseka😂😂😂😂😂😂 iweyo ndi wani

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 2 місяці тому +1

    😂😂😂😂😂 malawi ndife makape timaopa muthu ot tamuvotela tokha

  • @richardkumbambe-tg9qi
    @richardkumbambe-tg9qi 2 місяці тому +2

    Great indeed. Let's all rise ip.

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z 2 місяці тому

    ❤❤❤❤smdc

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 2 місяці тому +1

    Mr Bon Kalindo on fire 🔥🔥💪

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 2 місяці тому +1

    Kkkkkk wapolice samwa ambuye nditengeni

  • @JaneMzengeza
    @JaneMzengeza 2 місяці тому

    Mulungu azikutetezera nkhondo mukuimenya

  • @shamimmahomed6709
    @shamimmahomed6709 2 місяці тому +1

    Bon kalindo yemweyo kuti wawawa!!!

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 2 місяці тому +1

    😂😂😂 koma ndaseka DC ayi taa sikusinja Kodi

  • @fatsanibanda5213
    @fatsanibanda5213 2 місяці тому +1

    Yes iweeee ing'alure basi😂😂

  • @AlexanderBilliat
    @AlexanderBilliat 2 місяці тому

    The DC!!!!!!!!!!!!!!!

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow 2 місяці тому +1

    kkkk koma chimwana chakwa njedza kkk

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 2 місяці тому +1

    🤣🤣🤣🤣🤣 ngati Malawi ndiwandani Mr DC

  • @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un
    @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un 2 місяці тому

    Bon kalindo tili limodzi

  • @GiftFrancesco
    @GiftFrancesco 2 місяці тому +1

    The Dc ❤❤❤❤

  • @SamboRuphan
    @SamboRuphan 2 місяці тому

    Osafowoka bon kalindo

  • @KondwaniNguleti-x1q
    @KondwaniNguleti-x1q 2 місяці тому +1

    😂😂😂😂 Mr DC

  • @PeterMoosa
    @PeterMoosa 2 місяці тому +1

    More fire mr winiko

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 2 місяці тому +1

    Make mbuuu mwana mbuuuu 😅😅😅

  • @AlexNkhata-c8n
    @AlexNkhata-c8n 2 місяці тому

    Zoona akunena B kalindo

  • @thandothando6556
    @thandothando6556 2 місяці тому

    Super super😂😂

  • @kondwanijuwa-q4r
    @kondwanijuwa-q4r 2 місяці тому

    Koma iwe ndigalu kwambili

  • @RabsonSabit-nc5ds
    @RabsonSabit-nc5ds 2 місяці тому

    Uyu ndi nyoooo

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu 2 місяці тому

    Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1

  • @FlorenceMkandawire-w1m
    @FlorenceMkandawire-w1m 2 місяці тому

    Muma tiimila osatopa

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 2 місяці тому

    Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo

  • @ThokozanNyankhonde
    @ThokozanNyankhonde 2 місяці тому

    Umakwana iweyo

  • @HanifaIbrahim-o5u
    @HanifaIbrahim-o5u 2 місяці тому

    Hahaha kwachema 🔥

  • @Chipilirodaniel1989
    @Chipilirodaniel1989 2 місяці тому

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 місяці тому

    Bwana apolice atraffic akuonjeza bwerani mnseu wa Bunda every 200m atraffic ndie a area 3 amabwera 3koloko am kuyimba pa mnseu mmmmmmm Malawi

  • @JohnZyambo-q8h
    @JohnZyambo-q8h 2 місяці тому

    ❤❤

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 2 місяці тому

    Ipondeni Fadah

  • @AdiniKhama
    @AdiniKhama 2 місяці тому +1

    Mr DC osafowoka

  • @lawrenceblacktealyson8015
    @lawrenceblacktealyson8015 2 місяці тому

    I don't want to be Malawian anymore

  • @JohnZyambo-q8h
    @JohnZyambo-q8h 2 місяці тому

    🎉

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 2 місяці тому

    aaaaa zayambika liti tchega omwewu gati mwatopa nawo phandowo apatseni ena MCP is very nonsense iyaaa

  • @griviniakanjaula4456
    @griviniakanjaula4456 2 місяці тому

    More fire mbuyanga alomwe alomwe nophiya

  • @frankdonovanntambira
    @frankdonovanntambira 2 місяці тому

    Ndipo Boma Lamanyi ngati ili ine sindinalionepo Aaash!!

  • @PachaloShaba-pf5vw
    @PachaloShaba-pf5vw 2 місяці тому

    Good boy

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu 2 місяці тому +1

    Koma ndiye mwafikapo mpaka kulesa anthu kuti asamavuule mchenga really? Nyumba zanuzo munamangila mchenga munakawoda ku America? Silly people

  • @MemoryKamanga-jv4jh
    @MemoryKamanga-jv4jh 2 місяці тому

    You are welcome Mr dc

  • @KennethMchenga-j9c
    @KennethMchenga-j9c 2 місяці тому +1

    Pliz a DPP tadzukani kodi mukunafuna amalawi atani

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 2 місяці тому +1

      Ndipo zomwe akupanga a Dpp akumabowa kwambiri anthu akuzunzika ndi boma Koma aliphee ngati akumetedwa

    • @IbrahimYusufu-z9d
      @IbrahimYusufu-z9d 2 місяці тому

      Akufuna tidziwe kut tidapanga mistake.. ankatiuzatu paja

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 2 місяці тому

      @@IbrahimYusufu-z9d ndiye bola akazaluzanso asazalile chifukwa agalu a MCP akuwatakatu osusawa

  • @scoltenroma6240
    @scoltenroma6240 2 місяці тому +1

    Kuswa kuswa😂😂 akavote ndiamawo Oh yes 🔥🔥

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 2 місяці тому

    Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp palibe audio olo imoz inakambapo za Mr usi

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 2 місяці тому

    Kulephera kuja ndi kumeneku, anthu ndi okwiya kale , atopa ndi boma ili

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 2 місяці тому

    A opposition zochita zamwo ndi zimodzimodzi

  • @JasperKaleni-dx6nn
    @JasperKaleni-dx6nn 2 місяці тому

    😂😂the dc

  • @van-wykchilapondwa6981
    @van-wykchilapondwa6981 2 місяці тому

    Great 👍

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 2 місяці тому

    Kodi achakwerawa mchiyani makamaka zikuyenda koma??

  • @stevejizaremu3396
    @stevejizaremu3396 2 місяці тому

    The DC

  • @RichmanNkhoma
    @RichmanNkhoma 2 місяці тому

    Mbambande me. Kalindo

  • @irenioeugeniosumila6647
    @irenioeugeniosumila6647 2 місяці тому

    Ulemu wano A Kalendo

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds 2 місяці тому

    Eeeee koma ationjezadi apa ndiye yalakwa,,
    Tipindilana ndenvu mkamwa ulendo wake ndi umeneu

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 2 місяці тому

    Atsala atigulitsa mphweyaa kwatsala

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 2 місяці тому

    Mitu singwiradi.anthu onse anafa aja mwanzi wawo sukhara chete.

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr 2 місяці тому

      Mwazi unja wakuchingawa ukuwayenda Mitu anthu amenewa mchenga wobwela ndibvula 😅😅😅😅

  • @TapiwaKhwisula
    @TapiwaKhwisula 2 місяці тому

    Mo faya mr dc

  • @SilenceChepiano
    @SilenceChepiano 2 місяці тому

    DC ndimava kukoma mukatiyimilira

  • @StanleyChirwa-d6b
    @StanleyChirwa-d6b 2 місяці тому

    Koma Chaka chamawa tikhapana ndithu

  • @FrancisChimwaza-t7d
    @FrancisChimwaza-t7d 2 місяці тому

    Iswani ndithu man wamkulu ndi mulungu basi

  • @FrankiePangan
    @FrankiePangan 2 місяці тому

    😢😢😢😢

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh 2 місяці тому

    Ndkhulupilira kut a Malawi mistake iyiyi sitizachitanso

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 2 місяці тому

    Anapha zake chifukwa chaudindo

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 місяці тому

    Bwana ine office kuno ku Lilongwe tikupita kokayang'anira mayeso koma no allowances 😅

    • @PeterChilombo-ou2cd
      @PeterChilombo-ou2cd 2 місяці тому

      kkk iwe usandiseketse no what?aa. wabodzaiwe

    • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
      @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 місяці тому

      @@PeterChilombo-ou2cd ok u can not believe it,maybe your side, koma kuno tili sanatipasebe za Theory subjects

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi 2 місяці тому

    The D C!!!!

  • @charitykalua8507
    @charitykalua8507 2 місяці тому

    The DC😂

  • @MarvGerald
    @MarvGerald 2 місяці тому

    Km inuyo mumakwana kkkkkkkk the Dc

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula731 2 місяці тому

    Ubwino wake a Chakwera omwe mukuwanenawo sakuyankhani nkomwe, mumangobwebwetuka zaziii ngat ufulu omwe mumamenyera anthu osaukawo umathandizapo kalikonse, tikungogonabe ndinjala ngat mumati mukayankhula apa mumatipatsa ndalama, phindu lanu ndichani, ine ndiye nsaname zimandinyasa izizi, palibe chomwe munthu wanzeru angayamikire pazomwe mumayankhulazi, coz maboma onsewa zochitika ndizimodzi palibeso wabwino apa, n zonse izizi zilibe nzeru, nanga mpunga souseg zimenezo zikankhale zoyankhulira anthu osauka kapena zangolowa zidani zanu?? Zopusa

    • @StanleyChirwa-d6b
      @StanleyChirwa-d6b 2 місяці тому

      Samayankhatu mosathepo mau ap😅😅😅

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 2 місяці тому

      IWEYO ndi opusa kwambiri ndi chakwera wakoyo ngati akutuma cadet mbuzi, ngati iwe ukidya ndi mcp usawanyase AMALAWI AKUVUTIKA , ndiye uzikayankhula mbwerera zako zankutuzo , ngati sizikusangalatsa amakutuma kuti uzimvera ndi ndani ulibe manyazi ? Cadet supit

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 2 місяці тому

      @@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala

    • @StanleyChirwa-d6b
      @StanleyChirwa-d6b 2 місяці тому

      @@isaacchiwaula731 inu musokosa mungosiya kuverako bas sizokakamiza izi boss

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 2 місяці тому

      @@isaacchiwaula731 iwe sungamakhale KUMBUYO kwa mcp ngati sukuona momwe dziko lavundira ndiye kuduka mutu kumeneko , usiyamitse mene chakwera amatenga boma linali motani ndiye pano zilimotani ? Ndiye timusiye chakera alamuleso lidzakhala dziko? Anthu adzakhala ngati ndani, tiyeni tiganizire ana omwe taberekawa tisakhale ngati a police ndi asilikali amene asankha kigwira ntchito ndi chipano malo moteteza malamulo adziko,

  • @BudaEarth
    @BudaEarth 2 місяці тому

    U na problematic

  • @JamilahChitulu
    @JamilahChitulu 2 місяці тому

    😂😂❤

  • @phillgatoma4857
    @phillgatoma4857 2 місяці тому

    😢😢😢😢😢😢

  • @RidsonChafulumirah-r2y
    @RidsonChafulumirah-r2y 2 місяці тому

    DC

  • @muneeladan8580
    @muneeladan8580 2 місяці тому

    Mafia

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 2 місяці тому

    DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr 2 місяці тому

      Zosantheka Brazil ndipo idzankhala yazikwanje zomwe² mwaphela saulosinever again MCP achimwene

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 2 місяці тому

      2030 mcp ikakhala mnyumba mwa kwanu zopusa anthu opanda nzeru ngati akukudyetsani ndiye muphe anthu chifukwa choti mukudya ndi mcp yakuphayo yankhanza zachibwana

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 2 місяці тому

    The DC