Kod CHAKWERA Wamwalira? tamvani izi

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 4 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 164

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 місяці тому +10

    Rest in peace 😂ngati zili Zowona, ife timawona ngati ndiwoposa Mulungu tu, amuyaya

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 3 місяці тому +6

    I dont wait msg say lessen that ...Any way rest in peace chikangawa go well ❤❤🙌🙌

  • @berlz12k
    @berlz12k 3 місяці тому +1

    Ndipo ther is no peace for the weaked ndipo sindingamvere chisoni munthu oipisisa Malawi muno uyu!..apite kumene olo ntamva kuti zatero ndizangoti “rip skc and 8pipo”..justice shall be served..Mulingo umene umamulinga nawo nzako naweso uzalingidwa omweo..ndipo munthu sungakhale ndimtendere dziko lonse kumakamba zoipa za iweyo never..mxiew

  • @ChifundoOsman-h8q
    @ChifundoOsman-h8q 3 місяці тому +6

    Ngat ndichoncho ai akapume watidyesa chiteze 😂😂😂😂

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe 3 місяці тому +5

    Dziko ndila yehova

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 3 місяці тому

    😂😂😂😂my people ✋ @kullu nafs malikul kitaba kkkk ayi xikomo washiyao wangalusa yakuona eee.

  • @Josephiriillovo
    @Josephiriillovo 3 місяці тому +1

    CHEERS CHIKANGAWAAAA AMBUYE KUMWAMBAKO CHONDE DULANI MOYO WA LAZARUS CHAKWERA PLZ GOD IN HEAVEN

  • @MjombaMoosa
    @MjombaMoosa 3 місяці тому +2

    Why mcp is hiding this store

  • @ZathuzomweBenitoBLP
    @ZathuzomweBenitoBLP 3 місяці тому

    Limpompo yonama makape😅😅😅😅

  • @GraceMasiye
    @GraceMasiye 3 місяці тому

    Asafe koma azingozuzika nd kudwala mesa amat Peter wathu ndi wokalamba😂😂😂😂MULUNGU mwini moyo wapanga zoziwa yekha😂😂😂😂😂

  • @Lydia-t4b
    @Lydia-t4b 3 місяці тому

    Ndayamba kukaika zokamba zanu a Ntanyiwa including Bakali Muluzi tv. Nanga munthu kudwala choncho angapange ma press ups chonchija

  • @MisoziPhiri-k1t
    @MisoziPhiri-k1t 3 місяці тому

    Ndizoonadi chilimawamwalira ine ndimaona ngatiiye ndimulungu😂😂 8:31

  • @KelvinMungomo
    @KelvinMungomo 3 місяці тому

    Komano ngati wamwarira zitisangarasa chifukwa athu amazuzika 😂😂😂😂😂

  • @RashidPiano
    @RashidPiano 3 місяці тому +1

    Ngat Sanafe ine ndituma Anthu Kt Akamaleze Mission Kuzinga Ngati Mbuzi

  • @paulmolowa2688
    @paulmolowa2688 3 місяці тому +2

    Dziko ndi la yehova ndi zozala zake zomwe. Kwa iye ku khale ulemerelo lero ndi nthawi zonse

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 3 місяці тому +4

    Chimwalire bas chimunthu choipa mtima 😢

  • @JohnEdson-x5r
    @JohnEdson-x5r 21 день тому

    Muyeso umene umamuyesa mzako mulungu amakuyesa oposa msikhu wake yense okumbila dzenje mzake adzagwelamo yekha

  • @ChrissWtness-e1z
    @ChrissWtness-e1z 3 місяці тому

    Azaweluza akha mlungu

  • @CHRISMWAMS
    @CHRISMWAMS 3 місяці тому +1

    Yawina 😂😂😂😂😂 watizuza kokwana

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 місяці тому

    Kkkkkkkkkkllkkkkk tiziona ndi ntanyiwa

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 3 місяці тому

    😂😂😂 athu angundika akuti 20 30 wooo 😮

  • @AsapangaSainet
    @AsapangaSainet 3 місяці тому

    Akhala President wakumalawi, oyamba kuchira ku Garden city

  • @besterlumbe4404
    @besterlumbe4404 3 місяці тому

    Tsitsani mbendera chikangawa watisiya🕺🕺🕺🕺chisangalalo chake kuposa chapa 1 january😂😂

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 місяці тому

    Ntanyiwa, ntanyiwa, ntanyiwa ndakuitana kangat ndi maboza ako kuyipa nkhope ndi mau omwe chitsiru Cha munthu

  • @DamianoYohane
    @DamianoYohane 3 місяці тому

    President or kaya ndindani akadwala asamapite kunja koma adzipita kuchipatala cha m'Malawi mommuno.

  • @ChrisEnos-to5uv
    @ChrisEnos-to5uv 3 місяці тому +1

    Zosatira zakuchingawa zayamba kufika 😊

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 3 місяці тому +1

    Akanamugoneka kuzipatala zakwathu konko kumene sakugurirako mankhwala iye waba ndalama zamalawi nanga anthu akumuzi akadwala apanga bwa

  • @JailosMwanza-c4j
    @JailosMwanza-c4j 3 місяці тому +1

    Iwe ndiwausilu umatinamiza

  • @KennethBilali
    @KennethBilali 3 місяці тому

    Ambuye chonde malidzan 100%😂😂

  • @clesheinvestments
    @clesheinvestments 3 місяці тому

    Zonama zonse mwalankhula umu.
    Chepetsani kutalitsa nkhani zonama.
    Mawa President akupita kukamenya Golf.
    Mwanya nayo mwakhaula

  • @Frederick-s4h
    @Frederick-s4h 3 місяці тому +1

    My country is not going well

  • @FrankFrancis-ch3xv
    @FrankFrancis-ch3xv 3 місяці тому +6

    Yes! We can confirm that here report from galden city tilimbe mtima basi Mikel usi has to appoint his vice president 😢

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 3 місяці тому +1

    Achakwera awona zokhoma kwambili chifukwa cha nkhanza zawo ndipo chakwera atafa lelo ineyo ndiye ndisangalala koopsa

  • @KelvinJpchimphepo-sh6nc
    @KelvinJpchimphepo-sh6nc 3 місяці тому

    Malawi ndimaziwa ine ameneyo 😂🤣

  • @AlexNjanje
    @AlexNjanje 3 місяці тому +1

    Achipatala chonde yesetsani kuno sitikumufunanso tikamupeza komweko watizumza munthu ameneyi kwakwana anthu 9 osalakwa ajaa mizimu yawo myokwiya anasiya anthu omwe amawathandiza Yesu ndi ambuyedi

    • @TrizaGeorge-q8w
      @TrizaGeorge-q8w 3 місяці тому

      😂😂😂 yomweo chikangawa satanic

  • @JohnEdson-x5r
    @JohnEdson-x5r 21 день тому

    Ayende ndithu watikwana

  • @Frederick-s4h
    @Frederick-s4h 3 місяці тому +2

    Dan lu waigwetsa mcp ndinyimbo

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe 3 місяці тому

    Kodi ku ungaku united nations meetings amakonda kulodza ma president athu à.kumalawi..Ndiye pano akamdzapitanso adzikakhala ku visitors lodge where they will be cooking and eating.and bathing alone..by theor own malawi cooks.amen.but not the wicked azungus doing or hosting them.

  • @WilliamMasula-cb1mg
    @WilliamMasula-cb1mg 3 місяці тому

    Yawa asaname ,,, pretoria ndi jozi ndika mtundatu komanso akulankhulamo angadziwe chani or ku Garden City ko angayandikire 🤣🤣🤣🤣

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 3 місяці тому +2

    😂😂😂😂😂😂 ndudikila apeleke report aboma ndipomwe ndi comment ok

  • @fionahrightonie3520
    @fionahrightonie3520 3 місяці тому

    Komatu ku UNGA uku anthu amapangako zinthutu,si amutharika a Peter nawonso zanja lakumazele lidafa that time amachokelanso ku UNGA komwekoso. Nde katemela wake nde waukalitu yomwe amalandila kumeneko.

  • @AngelinaNantima
    @AngelinaNantima 3 місяці тому

    Kodi anthu openga Inu Kodi munakhalabwanji?
    Dzanja LA agogo ako ndilo ladwala mxa

  • @TinkaKabawo
    @TinkaKabawo 3 місяці тому

    Kod chitedzechi chabwela bwanji ndi chakwela tiyeni tizidzilimbikila osamaloza chala munthu masiku omaliza ano kudzakhala njala basiiiii

  • @ChristinaPhalula-s6l
    @ChristinaPhalula-s6l 3 місяці тому

    Mzukwa umeneu watitopesa

  • @ChiukepochakuzgukaMunthali
    @ChiukepochakuzgukaMunthali 3 місяці тому

    RIP Mr Chakwela 😮😮😮

  • @robsontyg3928
    @robsontyg3928 3 місяці тому +1

    Pathako panu nonse a dpp, amene wamwalila ndi Peter mathanyula

    • @Josephiriillovo
      @Josephiriillovo 3 місяці тому

      KUMENYA KUGWETSAAAAAAA MUNYERAAAAA MUNYAAAA MA CADET AMAGAZIIII

    • @PraiseKawerama
      @PraiseKawerama 3 місяці тому

      Akufa nd m"bale wakoyo

    • @simeonbanda4240
      @simeonbanda4240 3 місяці тому

      Chafwa ichoo iwe😂😂😂

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 місяці тому

    RIP chakwera 😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @TachikoMwanamanga
    @TachikoMwanamanga 3 місяці тому

    Bola next life asakakhaleso president 😭

  • @JerryUnyolo-r4u
    @JerryUnyolo-r4u 3 місяці тому +4

    Koma ngati wafad kumwamba kidyele nyama

  • @SammyHasani-g8e
    @SammyHasani-g8e 3 місяці тому

    ⚰️⚰️💉⚱️⚱️🤲🤲

  • @khasimMusa-d3w
    @khasimMusa-d3w 3 місяці тому

    Makolo apita chkangawa woyeeeeeeee kkkkkkkkkkk

  • @MichaelKaerama-dd4bk
    @MichaelKaerama-dd4bk 3 місяці тому

    😂😂😂 chikangawa

  • @BrianPhiri-s7x
    @BrianPhiri-s7x 3 місяці тому

    AKAPUME CHAKWELA WANAMA NTHAWI YAITALI LA 10 LAFIKA 😂😂😂😂😂😂😂RSP

  • @OdettaLowrence
    @OdettaLowrence 3 місяці тому

    🎉RIP CHIKANGAWA

  • @PreciousBanda-j9p
    @PreciousBanda-j9p 3 місяці тому

    Chikangawa woyeee

  • @YasenYasen-q9g
    @YasenYasen-q9g 3 місяці тому

    Ayi zicomo zabwino soze😂😂😂😂

  • @eliasgondwe
    @eliasgondwe 3 місяці тому

    Ma Cadet mukhalabe choncho mpaka YESU adzabwela osapeza mtendele, mudazolowela kudya zodzipenta

  • @LimbanStephano-d6n
    @LimbanStephano-d6n 3 місяці тому

    🙆

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 3 місяці тому

    Utsi subuka popanda Moto HA lero ndachedwa ku NTCHITO,kodi kumudziko zikuti bwanji?😢

  • @MikePaulo-y1o
    @MikePaulo-y1o 3 місяці тому

    Pita yomweyo abwelele olo bakhili abwelele

  • @ChristinaPhalula-s6l
    @ChristinaPhalula-s6l 3 місяці тому

    Anakomoko bwanji sanamwalile amwalile

  • @HenryNanthuwa
    @HenryNanthuwa 3 місяці тому +1

    😢

  • @MikePaulo-y1o
    @MikePaulo-y1o 3 місяці тому

    Geyezi ndidzoona

  • @GedoleafGondwe
    @GedoleafGondwe 3 місяці тому

    Galu anadya nsima yanga,pano amwalira achita bwino amwalira.galuwe mzimu wako usawuse mmtendere.hehede ulu

  • @egretamalawi
    @egretamalawi 3 місяці тому

    😢😢😢

  • @MrThomas-j9d
    @MrThomas-j9d 3 місяці тому

    Alimoyo chikangawa koma kukumununkhula kusabwera

  • @AmosSimeon-i5i
    @AmosSimeon-i5i 3 місяці тому

    Akause mu mtendere tikampeza 2099

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 місяці тому +1

    Akuchedwa kufa nyani hule chigawenga ameneyo mbuzi

  • @ChimwemweSynoa
    @ChimwemweSynoa 3 місяці тому

    Wailesi yabodza kwambili

  • @ehinsupport3217
    @ehinsupport3217 3 місяці тому

    Mwagwa nayotu ma cadet apa. Bodza lija balalaa. Manyazi bwaa?

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni 3 місяці тому

    Km akachedza ndichilima bwino bwino?? 😂😂😂😂

  • @Chifundo-cg7xi
    @Chifundo-cg7xi 3 місяці тому +1

    Ngati ndizoonad ambuye tengeni bas

  • @AngollaMunembo-bs9ot
    @AngollaMunembo-bs9ot 3 місяці тому

    Ngati chilima anafa iye kulibwanji? Tikasake ku chikangawa naye

  • @Kasawalah
    @Kasawalah 3 місяці тому

    Achile asathawe zisankho

  • @yunusibraheem4446
    @yunusibraheem4446 3 місяці тому

    Ine sindingalile aaaaa

  • @rhodahjere8747
    @rhodahjere8747 3 місяці тому

    Chimwalire basi chimunthu choipa

  • @modiseusi4412
    @modiseusi4412 3 місяці тому

    Koma Makomenti mbweeeeee kukunena kut oipa,, enaaaa pamaliro po mukamva anali wabwino ayi abwino sakhalitsa chabwino.......

  • @CHRISMWAMS
    @CHRISMWAMS 3 місяці тому

    Km ineso zothela data dzina aaaa za ziiii afe ndilibe naye mission

  • @ShuqItwa
    @ShuqItwa 3 місяці тому

    Ngati wafa chikangawa akause muntendere chifukwa watinzuza a Malawi

  • @AnnaPhiri-b8t
    @AnnaPhiri-b8t 3 місяці тому

    Aganyu ama 2000 ndiomwe angadandaule

  • @MikePaulo-y1o
    @MikePaulo-y1o 3 місяці тому

    Ngati wamwalila akaphume sitimufuna galuameneyo

  • @NedsonBanda-i2c
    @NedsonBanda-i2c 3 місяці тому

    Kkkkkk km ndye yaaa mwayankhulatu man ohool olila akhale a MCP okha

  • @ThandiShandu-l6w
    @ThandiShandu-l6w 3 місяці тому

    Okumba dzenje agweramo Linda madzi kuti adutse umazisempha iwe mtanyura

  • @DanielDoctor-t3p
    @DanielDoctor-t3p 3 місяці тому

    Oh zonse nthawi kaya ali moyo kaya wafa akudziwa ndi mulungu

  • @MariamChipoka
    @MariamChipoka 3 місяці тому

    Apite watikwana

  • @horacechera6978
    @horacechera6978 3 місяці тому

    Koma tisayembekeze kuti atalowa wina kuti zinthu zingayende even atalamula abambo anu sangasinthe dziko ngati ulesi wake ukhale omapemphetsawu ayi

  • @AnitacapombaMacoa
    @AnitacapombaMacoa 3 місяці тому

    Choyipa chitsata mwini

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 3 місяці тому +1

    , Mabodza awa pano ai.

  • @yamikaniraphael4975
    @yamikaniraphael4975 3 місяці тому

    Apitebwino

  • @ChisomoBanda-jo4ix
    @ChisomoBanda-jo4ix 3 місяці тому

    Amwarire nde bwino amene adati phera chirima

  • @MerryMphande
    @MerryMphande 3 місяці тому

    Igwe Basi mbendela

  • @khasimMusa-d3w
    @khasimMusa-d3w 3 місяці тому

    Tiyamike mulungu

  • @KondwaniGumba
    @KondwaniGumba 3 місяці тому

    Alipo ndipo akharapobe mpaka wina achita manyazi 2025.

  • @CliftonPhiri-m8v
    @CliftonPhiri-m8v 3 місяці тому

    Mbole yache afe basi

  • @HabiboZimba
    @HabiboZimba 3 місяці тому

    Koma zilibwino kwambiri iiii ambuye ayakha pephero lamawi

  • @innocentkandulu2825
    @innocentkandulu2825 3 місяці тому

    Wasala Gesebelo ndi azilongo ache Chimwendo Banda ndi Kamajekete

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 3 місяці тому

    Kumenya kugwesadi😅

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 3 місяці тому

    Bambo asikono mwai wanu ndiumeneo

  • @FrankMankhokwe
    @FrankMankhokwe 3 місяці тому

    Ndiye tsopano poti zinali zabodza ndiye iwe amene ukuwerenga ma comment we summarisation yako nd8yotani

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 3 місяці тому

    Ndipo ngati sakumwalila m,sanga chilima ndi athu ena anawapha kuchikangawa aja asamusiye amukoke sangamulephele kumuko amwalile changu asatinyase ife