BON KALINDO WANG'ALULA AZIBUSA __5 February 2025

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 9 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 46

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute3839 5 днів тому +4

    I always support you just because you stand for the truth may God always be with you the DCCCCCCCCCCCCCC from mulanje southern Africaaaaaaaa malawi

  • @JosephMpokosa
    @JosephMpokosa 4 дні тому

    😂😂 Chilungamo chimamveka Pena ngati mwano kkkk

  • @ShukulaniMthipera
    @ShukulaniMthipera 4 дні тому

    Makwana Mr DCCCCC ulemu wanu

  • @mathewshauya
    @mathewshauya 4 дні тому +1

    Azibusa anakulodzani ndani koma?? Mene Malawi waonongekelamu kumalambila munthu zoona a ccap? Zooona

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 5 днів тому +1

    CCAP ndi amfiti Bon kalindo avala zoyera koma mkati mwa mtima ali akuda 🎉🎉🎉

  • @BertherMatiya
    @BertherMatiya 3 дні тому

    Chilungamo chiyende ngati madzi

  • @DysonYohaneChingwalu
    @DysonYohaneChingwalu 4 дні тому

    iwetu nde adakoza

  • @SaidiMilinje
    @SaidiMilinje 4 дні тому

    Mumakwana big

  • @GreysonLimula
    @GreysonLimula 4 дні тому

    Mitumbo yawo azibusa a nkhoma synod machende awo kutigulitsa ife kamba ka 10 million

  • @Dellingsmunthali
    @Dellingsmunthali 4 дні тому

    Azibusa adyera akakowa awapasa nthumbwana basi akut bwana zilibwino azibusa a ccap adyera omasangarara anthu akuvutika

  • @RuthOsman-m6x
    @RuthOsman-m6x 3 дні тому

    Thana nawoni mu tea Estate muli nkhanza aoneseni afisi amenewo

  • @BernardChikopa
    @BernardChikopa 5 днів тому +1

    Kodi azibusa bvuto lanu ndi chani,,,makamaka aaaa mbuye akuyendereni,,,thawi yokhala limodzi ndi apulezdent.yatha inuyo simukuona mene awonongera zithu muno Malawi nde mumakatani kumeneko....ntengo ukakhota ngakhale utakula simungaungole awa ndi anthu oyipa,,azibusa opanda masophenya...

    • @DanielGanizani-h8r
      @DanielGanizani-h8r 5 днів тому +1

      Azibusa aCCAP koma ndi chani,ndine wa ccap koma mukutichitisa manyazi kwambiri ndinu mimbulu eti ija amanena Ambuye wathu Yesu eti?dyelanitu Moto ukukuyembekezani posachedwa,mulibe manyazi poyenda ndizina la ubusa mukutchulidwalo?mulibe mantha ndi Mulungu chifukwa chani?asatanic inu ,mundilakwisaso ,Mulungu alowe ndi nkwapulo munyumba ya m'busa aliyense mwalowa ndalama ya mwaziyi,mdzina la Yesu

  • @JustinMakoka
    @JustinMakoka 4 дні тому

    Apa ndiye akunyazisa mipingo anthuwa palibe kukhulupilira opemphera Maka mazibusa onse

  • @chisomochawinga4905
    @chisomochawinga4905 5 днів тому +2

    Ndiwe kape

  • @kennedychinguwo1640
    @kennedychinguwo1640 4 дні тому

    Komano pa nkhani yobera anthu muma kampani,kuzunza powagwiritsa ntchito anthu mwakalavuala gaga ndi kuwapatsa malipiro ochepa,zakhala zikuchitika kwa nthawi yayitali ndipo maulamuliro onse akuyenera kudzudzulidwa posapangapo kanthu.
    All the past regimes have to take the blame.All the governments have never taken any company accountable when the citizens are being exploited by their companies.And surprisingly most of these companies are depended by govt

  • @Kamwachale
    @Kamwachale 4 дні тому

    Let the opposition register all fertilizer beneficiaries and find out from each if he or she received all two bags of fertilizer if not then all who were responsible to be accountable otherwise this is theft.

  • @MartinKapito
    @MartinKapito 5 днів тому

    Auncle bon kalindo mulungu aonjedzere masiku anu popanda inu amalawi titha. Ndibu yemwe mumatidzindikiritsa ndi kutiunira

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 5 днів тому

    Inuyo the DC ndiwakulu❤

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 5 днів тому +1

    Zitsiru za abusa

  • @juliussamson6212
    @juliussamson6212 5 днів тому

    MAZIMBUSA NONSE MUNALANDILA NDALAMA ZOTI MUZIWUZA ANTHU MA CHURCH INUYO KAYA MUKUDAMBA MACHIMO YA CHAKWERA NDIPO MUKAYANKHA PAMASO PA MULUNGU CHIFUKWA CHAKWERAYO ANASANKHA KUPHA CHILIMA MALO MOFUNA KUPITILIZA UDINDO NOKHA INU MUZIFUSE KUTI CHIFUKWA CHIYANI SATANAYI AKUTIPATSA NDALAMA IZI KODI TSGWILA NTCHITO YOTANI KOMA CHIFUKWA CHOFUNA KUTI CHAKWERA ASAKALANGIKE YEKHA PAMENE AKUGAWILANI NDALAMA YACHIPHIMBA MASO KUTI MUSAWONE PATALI NOSE INU MWALANDILA NDALAMA MWAMVOMERA KUTI MUNAPHA NAWO MR CHILIMA AMEN MU JESUS NAME AMEN

  • @YassinzaoZao
    @YassinzaoZao 5 днів тому

    The DC katundu zenizeni azibusa aminewa ndi mbuzi kwambiri

  • @AbrahamLLoyd-xb2xc
    @AbrahamLLoyd-xb2xc 5 днів тому

    Powerful message

  • @MosesChinyamula-b3g
    @MosesChinyamula-b3g 5 днів тому

    This is the truth ❤

  • @VictorMateyu
    @VictorMateyu 5 днів тому

    YOU DESERVE RESPECT

  • @ManuelMagombo-m2u
    @ManuelMagombo-m2u 5 днів тому

    A Nkhoma synod anthu awo akumva bwino boma ili. Ndi chifukwa anapita kukafunila Chakwera zabwino.

  • @OscarDavidBanda
    @OscarDavidBanda 5 днів тому

    Kuyankhula mopanda mantha

  • @cyplusmsunje5483
    @cyplusmsunje5483 5 днів тому

    DC munabwera kuzaimilira malawi

  • @WellingsChiona
    @WellingsChiona 5 днів тому

    Kalindo iweso ndi mbuli kwambiri .Chiyambire sunagawepo chimanga .keep on shouting

    • @codeoflife1398
      @codeoflife1398 4 дні тому

      Azigawa chimanga cha chani nanu inu....mutu okhotawo

    • @JudithKatungwe
      @JudithKatungwe 4 дні тому +1

      😂😂😂😂😂😂😂

  • @OscarKathumba
    @OscarKathumba 5 днів тому

    Dpp never again ndipo ulira zeni zeni, uli ndi zaka zina 5 ,ukulakhula zopusa zakozo

    • @samdiverson9733
      @samdiverson9733 5 днів тому +2

      Ulila ndiweyo pulpet wa chabe chabe

    • @PiterDeleza
      @PiterDeleza 5 днів тому +2

      Wopusa ndiiweyotu chifukwa ukuyikila kumbuyo zopusa.

    • @fridaylestar
      @fridaylestar 5 днів тому +2

      Bola inuyo zilibwino zikukuyenderani komatu akuyankhualazi ndizowona anthu akuvutika, nkhani si DDP nkhani si MCP or UTM nkhani ndi a Malawi akuvutika ndipo zintbu sizikuyenda mu dziko lathu lino.

    • @codeoflife1398
      @codeoflife1398 4 дні тому

      I think ndiwe osabala.

    • @samdiverson9733
      @samdiverson9733 4 дні тому

      @@codeoflife1398 mpaka mwapeza chipangizo zoyezera kusabeleka kwa anzanu tikumana September 🤣