AFORD AKUPEPHA UTM KUTI APANGE ALLIANCE- ZOMWE ZAYANKHULIDWA KU NSOKHANO

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 21 сер 2024

КОМЕНТАРІ • 66

  • @RachelDongolosi
    @RachelDongolosi Місяць тому +7

    Amen 🙏 mawu amphavu Mulungu akutetezeleni azitsogoleli amene mukuimila a Malawi osaopa Mulungu alinafe

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Місяць тому +3

    MTAMBO kakhaleni kunyumba...tinatopa nanu.AFORD SIYINGAWINE MWANA WAWUPANDU IWE..UMVE ZIMENEZI KOMWE ULIKO

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 27 днів тому

    Utm udf my vote

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 Місяць тому +1

    Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Місяць тому

    That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano

  • @marthaphiri3600
    @marthaphiri3600 Місяць тому +1

    Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Місяць тому

    Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤

  • @LuwisKaigwaze-gr6cg
    @LuwisKaigwaze-gr6cg Місяць тому

    Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Місяць тому +1

    UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance

    • @KikaImran
      @KikaImran Місяць тому

      You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies

  • @WatipaCawinga
    @WatipaCawinga Місяць тому

    Magufuli wathu kupoto

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Місяць тому

    Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @IshmailDukuturu
    @IshmailDukuturu Місяць тому

    Mbuzi iyi Timothy

  • @RobertGoliat-gt2qh
    @RobertGoliat-gt2qh Місяць тому

    Iwe Mtambo leka bodza unatiputsitsa padzana kulankhula ngt zamzeru kma sitingakhulupilire munthu ngt iwe

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Місяць тому

    Yambani zomwe mukunenazo musanalowe muboma ,kenako Anthu adzakhulupilila Kuti mukufuna kutukula dziko. Anthu Andale inu mumangotizunza,Anthu wovota kumabvutika inu Ana anu akuphunzila kunja

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Місяць тому

    Chihana is my vote

  • @josephgabriel1016
    @josephgabriel1016 Місяць тому +3

    Timothy sangatinamize for the second time.....

  • @jamessoko9480
    @jamessoko9480 Місяць тому

    Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.

  • @johnussenu2848
    @johnussenu2848 Місяць тому

    Utm and udf boma

  • @PeterPhiri-u7h
    @PeterPhiri-u7h Місяць тому

    MuKufuna alliance mukuopa chani

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Місяць тому +1

    Amen 🙏

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune Місяць тому

    Join

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff Місяць тому

    Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Місяць тому

    Munthu oyipisitsa mtima Timothy sitingakumvere

  • @user-rg9zc6eo2q
    @user-rg9zc6eo2q Місяць тому

    My vote afod

  • @user-bv8wo2fn4e
    @user-bv8wo2fn4e Місяць тому +1

    I hope if all mupoto must vote for AFORD

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 Місяць тому

      Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 Місяць тому

    Wabodz uyu
    Mumater mukamafun mavot
    Mumakhal ngat anthabwino
    Chilimanso amater
    Chakweranso amater

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Місяць тому

    Bomo ylo ❤

  • @ntombiunice8637
    @ntombiunice8637 Місяць тому

    Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera

  • @Dickies-mk8cd
    @Dickies-mk8cd Місяць тому

    Tiyeni tikavote mwanzeru mcp must go.

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Місяць тому

    Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Місяць тому

    Zimenezo2 zithera konko mwene

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Місяць тому

    Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Місяць тому

    🫡🫡🫡🫡🫡🫡

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Місяць тому +1

    I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Місяць тому

      Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Місяць тому

    Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa

  • @BwanaGD
    @BwanaGD Місяць тому

    Komatu mtambo munthawi ino ukanankhala chete kaye munalumbwa kwabili nthawi inja ife kukopeka nanu lero munagopita kukamuphetsako chilima inu kumabwerako ndiye muliena nthawi inoyo mukanadenkha kuyamba kulingalira pazomwe munachita aaa

  • @Donnex-gn2sf
    @Donnex-gn2sf Місяць тому +2

    Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Місяць тому

      Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 Місяць тому

    Move

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Місяць тому

    Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential

  • @Syakinongwa
    @Syakinongwa Місяць тому

    Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v Місяць тому

    Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta

  • @user-wk7ut7ld1x
    @user-wk7ut7ld1x Місяць тому

    Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip Місяць тому

    Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx Місяць тому

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @emmanuelsambo1158
    @emmanuelsambo1158 Місяць тому

    It was only SKC

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Місяць тому

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Місяць тому

    Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD

  • @MosesNyalugwe-ll8hh
    @MosesNyalugwe-ll8hh Місяць тому

    Maloto achumba

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Місяць тому

    Koma chaka chino ziliko ndithu.

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Місяць тому

    Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP

    • @spargomw
      @spargomw Місяць тому

      I agree with you 100%❤❤

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 Місяць тому

    Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂

    • @VungaQueen
      @VungaQueen Місяць тому

      Kkkk😂😂😂😂😂

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 Місяць тому

    Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?

  • @user-eh1gn1nj9d
    @user-eh1gn1nj9d Місяць тому

    Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu

  • @TiyesNayuma
    @TiyesNayuma Місяць тому

    Chitsilu iweyo you failed as a minister

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx Місяць тому

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Місяць тому

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk