WOLEMEKEZEKA INU ANTHU ENA ONSE A GULU LIMENELI LA MTHAWIRA SPIRITUAL MELODIES... INE MALAWI NZANU KUNO KU DZIKO LA CHILENDO LA SOUTH AFRICA MU MZINDA WA CAPE TOWN WESTERN PROVINCE OF SOUTH AFRICA NDIKULEMEKEZA YEHOVA MLENGI WATHU AMENE NDIYE MWINI MPHAMVU ZONSE... AKUTSOGOLERENI MU MAGANIZO, NZERU, MACHITIDWE ANU A MASIKU ONSE NDIPO AKUDALITSENI NTHAWI ZONSE CHIFUKWA CHA MAYIMBIDWE WOKOMA WOTERE ❤❤❤AMEN.
Very nice piece. I like your songs and came across this just yesterday but it has won my heart. May God bless the composer, producer, director and the entire choir. Glory be to God
WOLEMEKEZEKA INU ATSOGOLERI ABAMBO NDI AMAYI.... MTHAWIRA SPIRITUAL MELODIES... NDIMAKUPEMPHERERANI NTHAWI ZONSE CHIFUKWA CHA MAYIMBIDWE ANU WOKOMA WOTERE KUCHOKERA UKO KU MUDZI BLANTYRE (MALAWI) YEHOVA MLENGI WATHU AKUYANG'ANIRENI USANA NDI USIKU, AKUTSOGOLERENI MU MAGANIZO, NZERU, MACHITIDWE ANU A MASIKU ONSE, AKUDALITSENI NTHAWI ZONSE.. ❤❤❤AMEN.
WOLEMEKEZEKA INU ANTHU ENA ONSE A GULU LIMENELI LA MTHAWIRA SPIRITUAL MELODIES... INE MALAWI NZANU KUNO KU DZIKO LA CHILENDO LA SOUTH AFRICA MU MZINDA WA CAPE TOWN WESTERN PROVINCE OF SOUTH AFRICA NDIKULEMEKEZA YEHOVA MLENGI WATHU AMENE NDIYE MWINI MPHAMVU ZONSE... AKUTSOGOLERENI MU MAGANIZO, NZERU, MACHITIDWE ANU A MASIKU ONSE NDIPO AKUDALITSENI NTHAWI ZONSE CHIFUKWA CHA MAYIMBIDWE WOKOMA WOTERE ❤❤❤AMEN.
Very nice piece. I like your songs and came across this just yesterday but it has won my heart. May God bless the composer, producer, director and the entire choir. Glory be to God
So inspiring
Yehova ndinu thanthwe langa ndipothawira panga kulibeso kwina komwe ndingapite
Mthawira nyimbo zanu ndimazikonda kwabas,
Bwanji kut muposite yija ya *mtendere*
A nice song very touching
The song simply means that : JEHOVA (THE ALMIGHTY GOD IS MY REFUGE AND MY ROCK!!!
WOLEMEKEZEKA INU ATSOGOLERI ABAMBO NDI AMAYI.... MTHAWIRA SPIRITUAL MELODIES... NDIMAKUPEMPHERERANI NTHAWI ZONSE CHIFUKWA CHA MAYIMBIDWE ANU WOKOMA WOTERE KUCHOKERA UKO KU MUDZI BLANTYRE (MALAWI) YEHOVA MLENGI WATHU AKUYANG'ANIRENI USANA NDI USIKU, AKUTSOGOLERENI MU MAGANIZO, NZERU, MACHITIDWE ANU A MASIKU ONSE, AKUDALITSENI NTHAWI ZONSE.. ❤❤❤AMEN.
Powerful
Very touching song
Nice song
Since 2020 I'm still watching this I don't understand the language bt I like the way
Praise be to God no where to go no where to run indeed only to God. Am humbled 🙏🙏🙏🙏
Good songs
ilike this Choir to be honest.....taponyani album yoyamba pls called Ntendere.
2023 still watching
Mumakwana takunyadilani
Zikomo Mr ngati palizina tumizani timakunyadirani Mr👏👏👏👏👏👏👏👏👏
Thanks guys for listening
Tikuthozeni anzathu mulungu akudalen chifukwa chamayimbidwe anu auzimu
Palibe zasopano?
Amen zili bwn zamphamvu mkokoma kuyimbira mulungu
Zilibwino koposa
Glory to God
Nice video special and perfect song🌹🌹❤️👍🙏
Please bweresani zambiri za Anthu awa amandidalisa kwambi
Good one
God bless you malawian my African
Super
Where is old guys I see new
Sikefa wefu wefu satopa
Amen
Zilibwino, koma za kale zija zili kut I tikuzifunanso chonde
Beautiful Gospel music 🎶
Great guy's .keep it up
Thank you so much
Ndathokoza Kwa mbiri
Mumatiimira guys may all mighty God bless you and add more skills upon of you 🔥🔥🔥🔥
Dgsryy
I miss home
Wawooooo
Tikuthozeni anzathu mulungu akudalen chifukwa chamayimbidwe anu auzimu
Palibe zasopano?
Nice song